Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1288 Yesu mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 669 Anyamata limikani,
  • Hymn 860 Nthawi yina adzadzuka
  • Hymn 46 INALIPO nthawi,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 239 TILI ndi mtendere
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 362 Imvani Yesu akuti:
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 1149 Chete! Chete!
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 653 Nditsogolere m’njirayi
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1112 Masiku anga onse
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 9 Mpingo woyera wa kwa anthuonse
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1434 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version