Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

  1. Home   »  
  2. Hymn 468 NDIKONDWA kuti

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 468 NDIKONDWA kuti

 

NDIKONDWA kuti
Atate wa M’mwamba,
Atidziwitsa chikondi chakecho;
Ndimaŵerenga m’Uthenga Wabwino,
Kuti Ambuye akonda ana ‘ke.

Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Yesu akonda, andikondabe;
Ndikondwa kuti Yesu akonda,
Amandikondabe.

Yesu ndim’konda, akondanso ine,
Anandifera pamtanda woopsa;
Wosayenera, woipa ndi
Tsoka langalo Ambuye nachotsa.

Mzimu Woyera akhala mwa ine,
Atsimikiza chikondi cha Yesu:
Ine n’tachimwa amandikumbutsa,
“Lapa mwana we akukonda Yesu.”

Ndikadzawona Ambuye Kumwamba,
Sindidzawopa pokhala akonda:
Anandikonzera kalelo nyumba,
Ndidzakhalamo wokondwa, wokoma.

Post navigation

Previous: Hymn 467 NGOLIZO zilira
Next: Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1089 Ndionetsere kuunika
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 61 Ndi chimwemwe ndimaona
  • Hymn 1569 Mtima wodetsa mukonzere,
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 1707 Andiferatu ‘Ye,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 171 M’manda munalibe
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version