Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
Next: Hymn 375 YESU m’khale nafe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 316 NDAMVATU kuti tifika komweko
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 985 Zonse zapadziko
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 910 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 419 ANYAMATA a Mulungu,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1642 M’khola mwa ng’ombe ku Betelehemu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version