Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 374 NDI lokoma m’Mwambamo,

 

NDI lokoma m’Mwambamo,
Mbuye, Bwalo lanulo;
Ndi mwabwino muli ’Nu
Dziko losachimwali;
Mtima wana wonsewu
Umakhumba m’Mwambamo
Nkhope ya Mbuyathuyu,
Mlungu wa chisomoyo.

Zimbalame zonsezi
Zimayamikira ’Nu;
Anthu amakondwanso
Okhumbira m’Mwambamo;
Njiŵa yosapumayo
Inafika m’chombocho;
Okhulupirira ’Nu
Amapuma kwanuno.

Anthu opembedzawo
Amakondwa m’mtimamo;
Munapatsa madzitu,
Munagwetsa manawo;
Mumakoma mtimatu
Tidzayamikiratu,
Pachimpando chanucho
Mkhale Mfumu yathudi.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 210 PEREKANI mtima wanu,
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 856 Kuunika kuoneka
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 867 Akristu ndi abale, tiziyenderana tonse,
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 1244 Nthawi ilikudza yonse
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 115 NTHAWI ija ya Sauli,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 212 Onse am’Mwamba ali mowemo,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1183 Adalitsika, indetu,
  • Hymn 984 Mpingo wa Mulungu
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1821 Angelo amazinga nyumba
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version