Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

 

KULI dziko labwino M’mwamba,
Lakuwala koposa dzuwa;
Yesu watikonzera malo,
Pokhalira ife komweko.

Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija;
Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija.

Tidzayimba komweko nyimbo,
Za abwino omvera Yesu;
Sitidzamva chisoni ife,
Tidzakondwa masiku onse.

Tidzatama Atate wathu,
Kuti Iye ‘napatsa Yesu;
Kuchotsera zochimwa zonse,
Ndikutidalitsatu ife.

Post navigation

Previous: Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
Next: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 825 Mpatse ana ‘ng’ono
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 34 AMITHENGA a Mulungu,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 1839 Yehova ndiye Mbusa wanga sin’ngasowe konse;
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 932 Munabvala thupi lathu,
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 770 Atate, muwapenye
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 935 Mtima ukachita nkhawa
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 150 Ndisauka, sindiona;
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 168 Yendani mwaulemerero,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 1260 Yesu, mulikundipempha, Munaterodi:
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version