Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

  1. Home   »  
  2. Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire

 

MBUYANGA Yesu, mundigwire
Dzanja.
Kuyenda ndekha sindikwana ’yi;
Mukandigwira dzanja langa, Mbuye
Sindikaopa kanthu kena ’yi.

Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
Pafupi ndi ’Nu nthaŵi yonseyo;
Ndikasoŵatu Inu, Mpulumutsi,
Ndingosekera m’talimo.

Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
Ukadza mdima m’mtima mwangamu;
Koma ndinutu dzuŵa langa ndithu
Lakuwalitsa m’mtima momwemu.

Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
Pamene ine ndimwalirapo.
Mkhaletu m’fupi nthaŵi yomwe Mbuye,
Mundiloŵetse ine m’Mwambamo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 431 Pompano pandikonda
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 964 Kodi simuona njira,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version