Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 281 Atate, ndipempha
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 195 Bwinoli tipita,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1806 Nowayo anatuma,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1802 Mulungu anatuma,
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1249 Tsirizani ntchito yanu
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 991 Ndi zapansi pano
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 866 Pa la Mulungu tibwera kulandira zidazo;
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1354 Mzimu Woyera, m’mtimamo
  • Hymn 528 Amithenga ‘naimba pamlengapo,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1094 Ambuye anachoka
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 989 Yochita ndi yodikha
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 416 PALIBE wina Kumwamba,
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 540 Amithenga akumwamba
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 1704 Zintchito zakezi
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version