Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

  1. Home   »  
  2. Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo

 

MUSAŴALOLE mawuwo
Apite ngati mphepozi,
Musaumitse mtimatu,
Polira Yesu Mbuyedi.

Idzanitu, idzanitu,
Idzani kwa Ambuyeyo.
Idzanitu, idzanitu
Apulumutse inunso.

Musachitenso nthantha ’yi,
Mufulumire inutu;
Tsiku labwino nleroli,
Mulandirenso moyowu.

Zokondweretsa m’dzikomu
Nzosakhutitsa m’mtimamu,
Koma za Yesu zonsezo
Zikwaniritsa inudi.

Sakukanani Yesudi,
E, mukalapa m’mtimamo;
Lolani kuti Mzimuyo
Agwire ntchito zakezo.

Post navigation

Previous: Hymn 146 KODI ulikulemedwa
Next: Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 401 Dzuwa la lero lonseli
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 1701 Nditani Bwenzi langa
  • Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 427 AULENDO amayenda
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 377 ANTCHITO a Mulungu ’nu
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1062 Mkatero ndidzayenda m’njira
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 622 Tiyamikira ‘Tate,
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 348 Aitana,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 1175 Sindinanyengedwa konse,
  • Hymn 1366 Sititha ifedi
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1201 Kumwamba kwanuko
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version