Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

  1. Home   »  
  2. Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,

 

KONZA mtima iwe mbale,
Pakuleka tchimo;
Siya zonse uzikonda,
Ndikutsata Yesu.

Konza mtima wako lero,
Yesu alowemo;
Ndipo usachedwe iwe,
Taata Yesu lero.

Imva kuyankhula kwake,
Mawu a chikondi;
Ayankhula iwe lero,
Kuti upumule.

Nthawi ya chisomo m’dziko,
Ndi inotu mbale;
Yom’dziwatu Mpulumutsi,
Ukali ndi moyo.

Post navigation

Previous: Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
Next: Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 836 Kamoyo kanga katha lero lino,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1063 Pokhala mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 270 Zoopsya zopambana
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 367 MPULUMUTSI, tikagona
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 443 Tchimo musalole,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 266 MBUYE ndamva mwawazira
  • Hymn 1837 Mbuye ndiye wachifundo,
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 152 Inde, Yesu, mundikonda,
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 36 Nyengo ifika, chenjera!
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version