Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

 

MTIMA wanga ndikonzera,
Mbuye Yesu aitana;
Ati: “Mwana, tapemphera,
Ine sindidzakukana.”

Mbuye ndinu Mfumu yanga
Yolemera ndi yamphamvu;
Ndikapemphatu zambiri,
Simundimanira kanthu.

Ndikabwera nd katundu
Wa zoipa zanga zonse;
Mwazi wake wa Ambuye,
Udzandiyeretsa konse.

Mbuye ndinalema ine,
Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Mkhale m’mwemo mwini wake,
Mantha mwandichotsera ’ne.

Ndine mlendo pansi pano,
Mndilimbitse ndi chikondi;
Bwenzi mundilondolere
Njira pa ulendo wonse.

Mndidziŵitse ntchito yanga,
Mphamvu yake mundipatse;
Mundilimbikitse m’mtima
Ndikhale kwa Atate.

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 279 Mbwere mudzamve nonse
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 828 Ndidzukanso m’mawa,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 414 Ana ake adzapuma
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1725 Zochimwa zanga zonsezo
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 509 Ndikadzaona Ambuye Kumwamba,
  • Hymn 324 TIKAGWIDWA ndi chisoni,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 72 Mayi watsogola ku Ulemerero,
  • Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 47 YESU panjirayo,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 1709 Pamtandapo Ambuyeyo anafera ifetu,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 399 Tchimo lathu lonse, Yesu,
  • Hymn 1103 Ndakudani, mnandikonda
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version