Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,

 

MTIMA wanga ndikonzera,
Mbuye Yesu aitana;
Ati: “Mwana, tapemphera,
Ine sindidzakukana.”

Mbuye ndinu Mfumu yanga
Yolemera ndi yamphamvu;
Ndikapemphatu zambiri,
Simundimanira kanthu.

Ndikabwera nd katundu
Wa zoipa zanga zonse;
Mwazi wake wa Ambuye,
Udzandiyeretsa konse.

Mbuye ndinalema ine,
Mloŵe Inu m’mtima mwanga;
Mkhale m’mwemo mwini wake,
Mantha mwandichotsera ’ne.

Ndine mlendo pansi pano,
Mndilimbitse ndi chikondi;
Bwenzi mundilondolere
Njira pa ulendo wonse.

Mndidziŵitse ntchito yanga,
Mphamvu yake mundipatse;
Mundilimbikitse m’mtima
Ndikhale kwa Atate.

Post navigation

Previous: Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
Next: Hymn 340 PEMPHERA m’mbanda kucha,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 614 Adzabwera Mbuye wathu
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 274 E! tidzakomanansotu
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 453 A! MULUNGU
  • Hymn 326 Yesu, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 418 M’manja Yesu wanga
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 183 Mlemekeze, bukitsani,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 1845 Zabwino ndi zokoma zinditsata chitsatire;
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1339 Musaope pokumbuka
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 1202 Ndikhumba mtimawo
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 760 Usiku uja kalelo
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 1326 A! Mbusa wathu amvatu
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 877 Zokoma ndithu nthawizi
  • Hymn 161 LERO lino mbale wanga,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 164 WANENA ndi Yesu,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 396 Mtitsogolere nthawi zonsezo;
  • Hymn 537 Aleluya! Aleluya!
  • Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version