Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,

 

KULI dziko labwino M’mwamba,
Lakuwala koposa dzuwa;
Yesu watikonzera malo,
Pokhalira ife komweko.

Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija;
Bwinoli tipita,
Tikomana mwa dziko lija.

Tidzayimba komweko nyimbo,
Za abwino omvera Yesu;
Sitidzamva chisoni ife,
Tidzakondwa masiku onse.

Tidzatama Atate wathu,
Kuti Iye ‘napatsa Yesu;
Kuchotsera zochimwa zonse,
Ndikutidalitsatu ife.

Post navigation

Previous: Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
Next: Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 166 NDICHITENJI kukapeza
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 915 Mumzinda wa Mulungu
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1533 Ndipatsa inu mtimawu,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 427 Komwe ndi chimwemwe
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1528 Naye Mzimu mndiphunzitse
  • Hymn 1030 Tioperanji ifetu?
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 1649 Kutenga inetu, kutenga inetu
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 521 Apunzitsi, ana omwe,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 976 Muyendenso kunka komwe,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 385 Tsopano, poyamba paja,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1086 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini moyo,
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 424 MTIDZUTSE, Mbuyetu,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version