Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

  1. Home   »  
  2. Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,

 

ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
Ŵalira Yesu m’ntchito zakozi,
Ŵalira Yesu pofanana ndi
Ambuyathu Yesu Kristu.

Tiŵaliretu, tiŵaliretu
Ambuye Yesu wotikonda ’fe;
Mlemekeze ’Ye tsiku lonseli,
Ine tiŵalire Yesu.

Ŵalira Yesu pazobvutazo,
Ŵalira Yesu pakukondwanso,
Ŵalira Yesu, imbirani ’nu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Ŵalira Yesu wolimbitsayo,
Ŵalira Yesu m’moyo monsemo
Ŵalira Yesu; tidzaonatu
Ambuyathu Yesu Kristu.

Post navigation

Previous: Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
Next: Hymn 178 ZAMBIRI zogona m’kholamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 1102 Dziko lonse ndilitaya;
  • Hymn 1146 Khalani duu! Pakufa mnzathuyo,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 63 POKUMBUKIRA mtandawo
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 135 Kudziwa ukudziwa,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 1563 Mufike monga nyali younika m’mtimamo,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1770 Iye amazichita zamphamvu
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 830 Atate ndiyamika, mwandisamalira leroli;
  • Hymn 1482 Tsopano inu ‘dzanitu,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 169 M’manda nagonamo
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 1577 “Kwa Iye atikonda
  • Hymn 1476 Mipingo iyo idzatu,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1491 Zokandweretsa m’dzikomu
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version