Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 930 Leroli chisoni chokha,
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 223 Ndafoka, ndaipa,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 1464 Nditama Nsembe ya Mulungu,
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 9 TAMANI Ambuye,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 69 KONDWERANI dzuŵa lino,
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1784 Komweko titasaukira,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 355 DZIKO lonse mlambire
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1040 Ukafuna kulemera,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 678 Ibukike mbiri yanu,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 862 Tidza kwa Mulungu Inu, ndinu wa chifundo;
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version