Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

  1. Home   »  
  2. Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,

 

USANABADWE, Yeremiya,
Ine ndinakudziwa;
Ndipo ndinakupatula,
Kuti ukhale mneneri.

Ulalike mawu anga Yeremiya,
Pita ukalalikire
Mawu anga;
Mawu anga Yeremiya.

“Usaopetu nkhope zawo,
Ine ndili ndi iwe;
Kuti ndikulanditsetu,
Iweyo,” ati Yehova.

Usaganize ndiwe mwana,
Iwe udzanka konse;
Kumene ndidzakutuma,
Kuti ukalalikire.

Post navigation

Previous: Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
Next: Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
  • Hymn 720 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1006 Yesu ati, “Ndidza msanga!”
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 1332 Imba kawiri ndi kawirinso,
  • Hymn 542 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 405 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1265 Tere moyo wanga wonse,
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 24 “Ndakupeza womanga,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 159 Kamwana Yesu ‘nabadwa,
  • Hymn 442 MASIKA a m’dziko Mbuye,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 37 Pozunzidwa inu ponseponsepo
  • Hymn 1794 Mulungu awakonda anthu
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 572 Anadza nazo mphatso zake
  • Hymn 330 N’LOKOMA Dziko langa!
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version