Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 1169 Mwazi wa Yesu
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1467 M’ulemerero mwake
  • Hymn 777 Mulungu ali muno,
  • Hymn 255 KHALA chete mtima wanga
  • Hymn 683 Musamaopa kanthu ‘yi, tamani Yesuyo;
  • Hymn 1742 Yesu ndinu moyo wathu,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 171 IWE tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1168 Aleluya, muyenera!
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 724 Ndine mlendo pansi pano,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1016 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 1076 Khalatu woyera,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 749 Ndiye wodyetsa anthu omwewo,
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1486 M’dziko lino pansi pano
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 627 Mlungu wathu mwatifitsa
  • Hymn 1543 Idzani, Mzimu Inu,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 300 AKRISTU limbikani,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1073 Mwa ine myatse moto wanu wakuyera mbuu,
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 118 Musaone zobvalazo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version