Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
Next: Hymn 106 MZIMU Woyera, mudzetu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 573 Ambuye, tikutamandani
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1033 Mkristu gwiratu ntchito
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1251 Ndasokera m’tali ndithu
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 468 Ife tikondana nanu,
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 343 ZOKOMA ndithu nthaŵizi
  • Hymn 551 Ndani kodi Munthuyo
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 322 Walira Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 959 Ana akumwamba ndife,
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 494 Yesu, E, ndikufunani,
  • Hymn 146 Inu ndidzatama
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 54 Dalitsani mafuko onse,
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 1746 Mwachimwemwe, mwachisoni,
  • Hymn 802 Ndife anthu aulendo,
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?
  • Hymn 1252 Pakukumbukira zanga
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 20 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1241 Ati: Mwana, kumbukira
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 846 Kristu wakuyeratu,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 226 BWENZI ndinamkomanayo
  • Hymn 1756 Mwana, adzakuyesa
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version