Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

  1. Home   »  
  2. Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

 

Yesu, dzina lakukonda,
Lopambana onse ena,
Tonse tidzaligwadira
Ndi mitima yochepetsa.

Yesu, dzina lokondwetsa
Akuipa a padziko,
Kale linatidziŵitsa
Mpulumutsi ndiye Yesu.

Yesu dzina lakufatsa,
Anamutcha ’kali Mwana,
M’mene analoŵa kale
M’dziko lino lakudana.

Yesu, dzina ndi lomweli
La pa dziko lino lonse,
Ndi lamphamvu yolanditsa
Anthu mu masoka onse.

Yesu, dzina lakukonda
La Mwanayo wa Mulungu,
Ife anthu osauka
Tithaŵira nalo kwanu.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1416 Mbuye wanga ndilikumva,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 657 Ambuye, ndi chikondi tho!
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 1029 Nkhawa tilibe; Yesuyo
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 286 ZOVUTA zoopsya ndi zosaukazi
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 271 Zoipa zangazi
  • Hymn 1460 Akuti anthu akumvera
  • Hymn 1827 Abramu kalelo anamvera bwino;
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 346 Aitana,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 328 Yesu ndiye mphamvu yanga,
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1116 Kwawo kwa Mbuyako
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 237 SINDINANYENGEDWA konse
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 1338 Munachita nthantha kale,
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 1436 Inde, lero lino Yesu
  • Hymn 455 Mdileke kulimbna ndi
  • Hymn 864 Ndi chikondi mtithandize kuigwira nkhondoyi;
  • Hymn 831 Mundikumbutse, ndikapanda tulo, za Kumwambako;
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 883 Pokupempherani
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version