Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 364 DZUŴA lapitira,

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 364 DZUŴA lapitira,

 

DZUŴA lapitira,
Wadza mdimawo,
Mthunzi wamadzulo
Wagwa m’mwambamo.

M’mwambamo nyenyezi
Zithwanima mbee;
Zonse zili m’tulo
Pansi pali duu.

Yesu mutipatse
Tulo toti phee;
Ndi mdalitso wanu
Mndigonetse ’ne

Mpatse ana ’ng’ono
Alotemo mbee;
Anthu aulendo
Msungesungebe.

Mutonthoze mtima
Wopwetekawo;
Akutsata tchimo
Mletse onsewo.

Wonsewu usiku
Andisunge ’ne
Amithenga anu
Akuyera mbee.

Ndidzukanso m’maŵa,
Kucha koti mbuu,
Ndiyeretu mtima
M’maso mwanumo.

Titamadi ’Tate,
Mwana wakeyo,
Mzimu Woyeranso,
Nthaŵinthaŵizo.

Post navigation

Previous: Hymn 363 ATATE ndiyamika,
Next: Hymn 365 DZUŴA lapita,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 1337 Bvomerani, Bvomerani,
  • Hymn 126 Mwa ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 381 Chakudya changa chabwino
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1606 Yesu, dzina lakufatsa,
  • Hymn 848 Mudze, mlowe m’mtimamu,
  • Hymn 826 Mutonthoze mtima
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 493 Ndimalira kwa Inutu,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 498 Yesu akonda,
  • Hymn 804 Muchotse zonse zoti bii
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 119 Tamverani anthu inu,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 342 BWENZI lathu ndiye Yesu,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 337 ‘Tate ‘Nu,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1314 Mulungu ali nane!
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 731 Mundionetse, Yesu,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1277 Kuti mukhululukira tchimo langalo
  • Hymn 714 Dzuwa ndi mvula yonseyo
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1384 Mphamvu yake inalenga
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version