Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 1727 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 142 Kukondwa kwa wodwalayo
  • Hymn 889 Pemphera m’mbanda kucha,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 102 MZIMU Woyera, mudzetu kwa ine
  • Hymn 1507 Ndikampempha anditenge,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 117 CHOLIMBITSA mtima ndi chonditsogolera;
  • Hymn 1412 Imfa idzafika msanga;
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 269 NDILIRA ine kukayenda
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 1564 Mufike monga moto wakuotcha zomwezo.
  • Hymn 921 Komwe Mbusa kwawoko
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 596 Mlungu ali nane;
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1553 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 510 Ngolizo zilira
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 314 E, moto wanu woyera

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version