Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 82 YANG’ANANI, anthu onse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 476 MBUYE, tili ana anu,
  • Hymn 778 Mwini madalitso,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 982 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 700 Mzimu woonadi
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 759 Ndilawako tsopanoli
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 997 Mawu ake atipatsa
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 373 Ayamikire ‘Nu
  • Hymn 1712 E! Yesu Mbuye wangadi,
  • Hymn 5 Inu Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 417 M’BWERE Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 142 MULUNGU aŵakonda anthu
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1828 Timtamande Iye ndi moyo wathunso
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 1536 Ndilira Mzimu leroli,
  • Hymn 1581 Ndi nyimbo yabwino
  • Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version