Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

 

MBUYE Yesu adzabwera,
Asekere anthu onse;
Mawu awa achimwemwe
Azimveka m’dziko lonse.
Adzabwera, adzabwera;
E! bwerani Mbuye wathu.

Dziko lino linaona
Masauko a Mbuyathu,
Lidzaonanso ulemu,
M’mene adzabwera Iye.
Adzabwera, adzabwera;
Timvomera, E! mubwere

Anthu anu amafoka,
Pa ulendo nasokera;
Ha! Adzaonana nanu
Atabvalanso zoyera.
Mudzabwera, mudzabwera;
Inde Mbuyetu mubwere.

Ndi chiyembekezo ichi
Sitikhala chete ife:
Tiimbitsa nyimbo zathu
Zakulemekeza Mlungu.
Adzabwera, adzabwera
E!! mubwere msanga YESU.

Post navigation

Previous: Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
Next: Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 1842 Pabande lolunjika andilondolera njira;
  • Hymn 147 Ndisauka, ndinachimwa,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1793 Pakuwoloka mtsinje wa imfa
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 1745 Yesu aitana ife:
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1083 “Khala mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 214 Msanga adzachitseka chitseko,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 575 Taonani m’kholamo
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 181 Zonse ndinakonda kale
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 464 AKAZI anadza kwa Yesu ndi anawo,
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 1783 Tinasokera ngati nkhosa,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 783 Antchito a Mulungu ‘nu
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 321 Ndi ponse paphiri ndi padambopo
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1608 Yesu, dzina lakukonda
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 912 Makomo afanana
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version