Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,

 

DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
Ndili ndekha mpanjira n’kwaŵenitu;
Ndilibetu chakudya, ndilibetu chakumwa,
Ndingoyenda mpanjira n’kwaŵenitu.

N’kwawenitu,
N’kwawenitu,
Dziko lino sikwathu
N’kwaŵenitu.

Dziko lino lapansi mavuto ndi osatha,
Ine sindingalithe n’kwaŵenitu;
Ukasowa chumacho, abwenzi akuthawa,
Koma kwathu satero n’kwaŵenitu.

Anyamata, ‘sungwana
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu;
Abambo ndi amayi
Samaopa Mulungu,
Sichifukwa chinanso n’kwaŵenitu.

Tiyeni abale ‘fe tiyang’ane kwa Yesu,
Yemwe angatipatse moyowotu;
Moyo uno wam’dziko abale ndi wozunza,
Moyo wokoma ndiwo wa Yesuyo.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1684 Mbuye mabala anu olimba
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 474 Yesu ndafikatu,
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 389 Ambuye, mtidalitsetu,
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1690 Titama Yesuyo,
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 803 Mulungu wanga, Dzuwatu
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 306 YAMBA ulendo mnzanga,
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 1258 Zonse zina sizikwana,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 219 YESU Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1666 Yesu, ndinutu chitsime
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 222 Ndilikudzatu,
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 795 Sitinanyalanyalaza
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1428 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1347 Akukonda, akukonda,
  • Hymn 1350 Mvera Yesu, mvera Yesu,
  • Hymn 412 Kudzachera tsiku lijalo
  • Hymn 425 Ine ndine mlendo
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 446 YAMIKANI nonse ’nu,
  • Hymn 328 KULIBE vuto
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version