Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1804 Mulungu anatuma,
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 391 Mufafanize m’bukumo
  • Hymn 293 LIMBA mtima mbale wanga
  • Hymn 1099 Sindidziwatu zamawa,
  • Hymn 455 TIIMBE ndi kulalikira
  • Hymn 696 Ufumu wake udalitsa
  • Hymn 650 Tikondwa tonse ndi kukuthokazani Nu
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 295 AMBUYE wa Kumwamba,
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 134 Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 988 Ndikhumba Mzimu wanu
  • Hymn 1555 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 729 Ndifuna kumva Inu,
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 407 Zochimwa sizilowako,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1615 Anakonda,
  • Hymn 1447 Yesu ngwachifundodi,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 1378 Tsopano linoli

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version