Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

  1. Home   »  
  2. Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 495 MLUNGU dalitsani Malaŵi,

 

MLUNGU dalitsani Malaŵi,
Mumsunge m’mtendere;
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje;
Lunzitsani mitima yathu
Kuti tisaope,
Mdalitse Mtsogoleri, nafe,
Ndi Mayi Malaŵi.

Malaŵi dziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m’mapiri,
Ndithudi tadala;
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Mphatso zaulere;
Nkhalango, madambo abwino,
Ngwokoma Malaŵi.

O! Ufulu tigwirizane
Kukweza Malaŵi;
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire;
Pankhondo nkana pa mtendere
Cholinga n’chimodzi,
Mayi, Bambo, tidzipereke
Pokweza Malaŵi.

Post navigation

Previous: Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
Next: Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 14 MTIMA wanga uyamike,
  • Hymn 981 Tiyeni Akristu,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
  • Hymn 368 Yehova ndiye Mlungudi,
  • Hymn 278 TITHAŴIRENJI ifetu
  • Hymn 127 Mwazi wake ndi chitsime changa,
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 1620 Aleluya,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 996 Leka zakuipa zako,
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 1327 Bwezatu, bwezatu,
  • Hymn 710 Nthano ya Hananiyayo
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 454 Kapena m’mtima ndimakwiya,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 1633 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 623 Mbuye, tikuthokozani,
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 768 Ndi ife tinga mbewuzo
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 878 Zokoma inde nthawizi
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 230 AMBUYANGA Yesu,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version