Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

  1. Home   »  
  2. Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

 

ONA Mwanawankhosayo
Wakuseza zakuipa zathu zonse.

Mwana wankhosa
Watisenzera
Zakuipa zathu zonse.

Anazenza m’thupi mwake;
Pakukhomedwa pa mtanda anali duu.

Ona pamtanda Yesuyo
Anabvutika chifukwa cha anthu’fe.

Imva kulira kwa Yesu
Pamene anasiyidwa muimfayo.

M’mwazi wake tisambamo;
Zichotsedwa zakuipa zathu zonse.

(Ona Mwana wa nkhosayo
Wakusenza zakuipa, zathu zonse.)

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 423 MUNENE Mbuye, ’nenetu,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 1305 Ndi ine pondibvutapo
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 928 Usalire; Mpulumutsi
  • Hymn 474 MPULUMUTSI, Mbusa wathu,
  • Hymn 422 DZIKO lonse lapansi,
  • Hymn 532 Ukondwere mtima wanga
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 838 E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 1085 “Khala mwa Ine,” ndinu mwini mphamvu,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1445 Tiyeni tonse, tinkeko
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 923 Dothili kudothilo,
  • Hymn 452 MLUNGU, Inutu,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1364 Uzani zamphamvu,
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 712 Mulungu akondadi leroli
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 163 Mukonda nyimbo za ana,
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 761 Natamndira Mlunguyo
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 545 Anatifera tonsefe
  • Hymn 189 Koma Iye wandipeza;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version