Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 229 POYAMBAPO ndakondwadi.
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 77 MMENE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 1682 Atha masiku aja ansoni,
  • Hymn 594 Monga may’ asusuza
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1618 Anakwera,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 272 Ankhondowo poona
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 628 E! chisomo chosaleka
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1587 Nditama Mlungu m’mtimamo,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 260 ODALA ndi onsewo,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 1343 M’dzina la Yesuyo
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1376 Akulu nonse ndi mafumu ‘nu,
  • Hymn 1098 M’mene mantha andigwira,
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version