Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

  1. Home   »  
  2. Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

 

TIANA ife tingofoka,
Sitikhala ’mphamvu ’yi;
Tikhoza kukachitiranji
Yesu kumkondwetsadi?

Tiana ta Ambuye tili
N’ntchito yaikuludi,
Kudzichepetsa ndi kusiya
Tchimo lili lonseli.

Kapena m’mtima ndimakwiya,
Nditukwana mnzangayo,
Kapena ndidzitama – izi
Ndilekere Mbuyeyo.

Ndileke kulimbana ndi
Kuŵanamiza enawo;
Ndinene zakufatsa,
Zakukondweretsa Yesuyo.

Tizikondana, tisekere
Tsiku lonse kwathuko,
Muyere m’mtima popeza
Yesu ndi Woyerayo.

Palibe mwana wakuchepa
Kunyamula mtandawu;
Ambuye Yesu mutipatse
Mtima wokondanatu.

Post navigation

Previous: Hymn 479 ANYAMATA inutu,
Next: Hymn 481 USACHIMWE konse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 172 Imfa yalephera
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 1026 Inde nditaya chumacho,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1751 Mbuye ngwodalitsika,
  • Hymn 1534 Mukonze mtima wangawu,
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 1471 Ukapenya kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 184 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 333 M’DZIKO lino tikhalamo
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1189 Ambuye Mulungu,
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 674 Anthu onse taukani,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 568 Taukani, taonani
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 546 Kulibe wokwanira ‘yi
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 698 Polenga dzikoli,
  • Hymn 221 Yesu and’itana,
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 793 Tikondwera kuti
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 287 Mitima yathu iyi nayo njanu,
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 194 Kuli dziko labwino m’Mwamba
  • Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 42 Masiku tikatsala ife
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 105 Tiyamike Mbuye Yesu
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 298 “Tadodoma, abusa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version