Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,

 

IMFA ya Mwana wa Mulungu,
Inali yomvetsatu chisoni;
Anatifera pa mtandapo,
Kutiwombola kumachimo.

Chinsalu cha m’kachisi
Chinang’ambika pakati
Ndi pempho la
M’dzina la! Tate,
Ndi Mwana ndi Mzimunso.

Mbuye Yesu ponka
Kumwamba,
Nanena, “ndikupita kwa “Tate;
Kukakukonzerani malo,
Ndipo Ine ndidzabweranso.

“Koma mudzalandira mphamvu,
Mzimu Woyera ‘tadza pa Inu”;
Ndipo tonsefe ndife mboni,
Kutitu Mzimu ndi Nkhosweyo.

Post navigation

Previous: Hymn 47 YESU panjirayo,
Next: Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 289 ANATILEMBA Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 445 TILIMALIMA m’minda,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 558 Mwanayo wa Mulunguyo
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 1767 Ndiye anayang’ana
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 1715 Kodi misozi itisowa,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 927 Pakutsazikana nanu
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 225 Yesu akhazika
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1107 Anthu onse pansi pano
  • Hymn 1825 Zobvuta zoopsa ndi zosaukazi
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 201 Ngati zakuipa zathu
  • Hymn 277 Mbwere nonse muone
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 701 Inu Atatuwo,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 904 Komweko akhala Yesuyo
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version