Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

 

MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali,
Nyenyezi, mwezi mbee,
Ndi dzikoli.

Koma ineyu
Simuiŵala ’yi;
Mundisamala ’ne
Ndisagwe ’yi.

Mbuye, Msungi ’Nu,
Mutuma indedi
Za moyo wangawu
Zokomazi.

Yesu Mwanatu
Anafa imfayo
Achotsa zoti bii;
Nadzukanso;

Kuti m’Mwambamo
Ndikatamandetu
Wondisamalabe,
Mbuyangayu.

Post navigation

Previous: Hymn 451 MLUNGU alinane;
Next: Hymn 453 A! MULUNGU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 1689 Dzukani nayetu,
  • Hymn 62 Tchimo lonse ligonjera
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 173 MWAMVA Mawu a Mulungu;
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 743 Mudze, anthuni, talawani ‘nu
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 352 NONSE okhala pansipa,
  • Hymn 1212 Zina ndi zinanso
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 609 Zanu zapansi nzokoma Mbuye; tikondwera ‘fe,
  • Hymn 1111 Pamene ndilemedwa
  • Hymn 853 Pa tsikuli, Mbuyanga ‘Nu,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 157 Mbuye, Mzimu Woyera
  • Hymn 1400 Tulani zoipazi, idzanitu,
  • Hymn 581 Mtiphunzitse bwinotu,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1480 Afika Yesu leroli,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 723 Mundimvere, Mbuye wanga
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 1316 Ndabwera kwa Ambuyeyo:
  • Hymn 4 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 283 Ndalema ndathodwa
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 1045 Ambuye, ndifuna nditsukenitu;
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 1353 Ambuye Yesu, Inutu
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version