Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 452 MLUNGU, Inutu,

 

MLUNGU, Inutu,
Mwalenga dzuŵali,
Nyenyezi, mwezi mbee,
Ndi dzikoli.

Koma ineyu
Simuiŵala ’yi;
Mundisamala ’ne
Ndisagwe ’yi.

Mbuye, Msungi ’Nu,
Mutuma indedi
Za moyo wangawu
Zokomazi.

Yesu Mwanatu
Anafa imfayo
Achotsa zoti bii;
Nadzukanso;

Kuti m’Mwambamo
Ndikatamandetu
Wondisamalabe,
Mbuyangayu.

Post navigation

Previous: Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
Next: Hymn 461 ANA inu, myamikeni

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 276 Dziko lonse mlambire
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 148 PAKUPEMPHA ife pano,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 185 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1566 Mufike monga ngati mphepo yokokomayo,
  • Hymn 487 Yesu, ndikabwera
  • Hymn 1452 Inu akutopawo,
  • Hymn 1077 Khalatu woyera,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 309 ANA akumwamba ndife,
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 357 Yesu ndiye Mtetezi,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 60 Chitetezo chachikulu
  • Hymn 435 ANAKWATIRA kale
  • Hymn 378 KWEZANI mitu yanuyo,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse
  • Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 977 Musagonje, anthu inu,
  • Hymn 14 Tsiku ndi tsiku timalemekeza;
  • Hymn 813 Wopulumutsa, Inunso
  • Hymn 757 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 437 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 386 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 482 TCHIMO musalole, musadziipitse,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version