Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

  1. Home   »  
  2. Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 309 ANA akumwamba ndife,

 

ANA akumwamba ndife,
Paulendo timaimba;
Timatama Mbuye wathu
Wa ulemerero wonse.

Tilikupita kwathu kuja
Munjira ya atate athu,
Amakondwera lero lomwe;
Tinka kuonana nawo.

Mbuye anatiitana
Kukagwira ntchito yake,
Kuitana anthu onse
Atsatenso njira yino.

Inde Mbuye, tibweradi,
Zathu zonse tizisiya,
Mtsogoleri wathu ndinu
Titsatabe inu nokha.

Post navigation

Previous: Hymn 308 AULENDO, munka kuti
Next: Hymn 310 MBUYE munditsogolere,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 278 Aweruza ndi mphamvu
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 56 Masiku onse timakondwera
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 939 Ambuye andisunga
  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 1776 Tiyeni timgwadire
  • Hymn 499 ‘Nafera Mbuye wanga
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 913 Kulibe gombe, nyanja,
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1109 Pamene ndisauka,
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 403 Dzuwa liwala, m’tulotu
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 1472 Ona! Ona! Onatu!
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 1002 Haya! ‘Nzanga taonani Yoonekayo
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 478 YESU atiuza tiŵale ’fe.
  • Hymn 1686 Ndi mtima wonse mwimbedi
  • Hymn 718 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,
  • Hymn 198 M’dziko lino tikhalamo
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 907 Dziko labwinotu, dziko labwinotu,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 472 YESU, ndikabwera
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1181 Adalitsika munthuyo
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version