Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

 

NJIRA yanga sindiziŵa,
’Tate muikonza;
Komatu muzindikira
Kuti mundikonda.

M’mene mantha andigwira,
Andidetsa m’mtima,
Mbuye, ndithaŵire kwanu
Poti mundikonda.

Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
Ndidzakhulupira Inu
Kuti mundikonda.

Inde wakukonda ndinu;
Mawuwo oona
Andidzaza ndi chimwemwe:
Mlungu andikonda.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 429 Haya! Tipitenso
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 1174 Sindinanyengedwa konse;
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 326 TSIKU Iidzafika mbale,
  • Hymn 709 Munthu aganize
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 1477 Anena anthu onsewo,
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 128 Yesu Mfumu, ine ndingadzafe
  • Hymn 524 Wokoma Mbuyathu
  • Hymn 268 Potuluka m’mudzimo
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 652 Munene Mbuye ‘nenetu,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 1271 Onani Mbuye ndigonja,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 39 Poyang’ana ena ndi ndalamatu,
  • Hymn 302 Anasenza m’thupi mwake;
  • Hymn 703 Dzuwa, madzi, kudya, mpweya,
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 1753 Adzatipulumutsa
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 1427 Penyetsetsa Yesu,
  • Hymn 202 Timpemphere kutipatsa
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version