Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

 

NJIRA yanga sindiziŵa,
’Tate muikonza;
Komatu muzindikira
Kuti mundikonda.

M’mene mantha andigwira,
Andidetsa m’mtima,
Mbuye, ndithaŵire kwanu
Poti mundikonda.

Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
Ndidzakhulupira Inu
Kuti mundikonda.

Inde wakukonda ndinu;
Mawuwo oona
Andidzaza ndi chimwemwe:
Mlungu andikonda.

Post navigation

Previous: Hymn 256 NGATI mtima sumakonda
Next: Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 1585 Dzina ili ndi lokoma
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 785 Yehova adalitse ‘nu,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 1192 Pamtanda woopsa
  • Hymn 1100 Inde wakukonda ndinu;
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 924 Kodi uli ndi chisoni
  • Hymn 684 Zipata zatsegudwa mbee! Za m’dziko monsemo;
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 475 Mbuye ndikhaletu
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 85 MASO ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 908 Ndikonda kuganizirabe
  • Hymn 1335 Wandifera Yesuyo
  • Hymn 1433 Lero lino ndi labwino;
  • Hymn 497 TILIKUIMBA nyimbo yomweyi,
  • Hymn 491 KWA Yesu ndi kwabwinoko,
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 140 Panalitu wakudwala
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 492 Yesu Mbuye ‘Nu wafatsa
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 807 Mpulumutsi tikagona
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 880 Bwenzi lathu ndiye Yesu
  • Hymn 790 Zimbalame zonsezi
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 434 Zondipingitsa zonse
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 248 M’MENE ine ndisauka
  • Hymn 195 YESU wondikondadi,
  • Hymn 76 Ndipereka zanga zonse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version