Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 257 NJIRA yanga sindiziŵa,

 

NJIRA yanga sindiziŵa,
’Tate muikonza;
Komatu muzindikira
Kuti mundikonda.

M’mene mantha andigwira,
Andidetsa m’mtima,
Mbuye, ndithaŵire kwanu
Poti mundikonda.

Sindidziŵatu zamaŵa,
Koma sindiopa;
Ndidzakhulupira Inu
Kuti mundikonda.

Inde wakukonda ndinu;
Mawuwo oona
Andidzaza ndi chimwemwe:
Mlungu andikonda.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 440 Yesu wakufatsa mtima
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 1590 Mtima ndimakondweramo,
  • Hymn 1226 Wandipatsa moyo wake,
  • Hymn 1007 M’mene umauka m’mawa,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 1607 Yesu, dzina ndi lomweli
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 46 O! ufulu tigwirizane
  • Hymn 771 Tsopano alandira
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1131 M’mene ine ndisauka
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 1499 Simbanitu mwachete
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 217 E! kwa Inu, E! kwa Inu!
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 1694 Timwimbire Mlungu wathu, Aleluya
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 899 ‘Tate wa Kumwambako,
  • Hymn 1242 Ku zoipa zonse zako,
  • Hymn 11 NDI mitima yokondwera,
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 469 Lero mkhale nafe ndithu,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu
  • Hymn 613 Dziko lonse nla Mulungu
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version