Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

  1. Home   »  
  2. Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,

 

MULUNGU anditsogolera,
Ndapumula m’mtimamo;
Ayang’anira njira zanga
Nsiku zanga zonsezo.

Mulungu anditsogolera
Nsiku zanga zonsezo;
Ndidzatsatira Mbuye wanga
M’njira mwake momwemo.

Masiku ena pali mdima,
Ndivutidwa m’mtimamo;
Masiku ena ndikondwera
Ndi zabwino zangazo.

Masiku onse m’mtima mwanga
Ndili ndi mtenderewo,
Chifukwa ndimakhulupira
Mtsogoleri wangayo.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 1797 Chikondi chake chindidzera
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 873 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 35 KODI mwaona chiyani,
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 138 SANGALATSA akusowa, masiku alikutha,
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 235 ADALITSIKA munthuyo,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1699 A! Mutu wakuyera,
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 1292 Wolapa mtima simunyozadi,
  • Hymn 64 LERO Kristu anauka,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 154 Pemphero ndiko kulira,
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 477 Mpulumutsi, Mbusa wathu,
  • Hymn 797 Kwacha lero kwati mbee,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 226 Nditama mwaziwo!
  • Hymn 1333 Idzatu kwa Yesuyo,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 491 N’takafika kwanu
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 112 ELISA mneneri,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 1785 Tiyeni tizipita kwathu,
  • Hymn 204 NDASIYA zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 1831 M’mitsinje yamtendere mtima wanga aumwetsa;
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version