Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

  1. Home   »  
  2. Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

 

TITAME Mlungu Wakumwamba,
Timwimbire nyimbo,
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo.

(Timwimbire nyimbo,
Timwimbire nyimbo!
Kukoma kwake kwatipatsa
Zonse tili nazo)

Poyamba paja analenga
Zonse dziko muno,
Tsopano lomwe azisunga
Zonse zili moyo.

Tinasokera ngati nkhosa,
Moyo tinataya,
Tinakondwera ndi zoipa
Zonse tinatsata.

Komweko titasaukira,
Titafuna kufa,
Atate anatilondola
Naitana ife.

Tiyeni tizipita kwathu,
Tisasokerenso,
Tilape m’mtima kuti
tikakhale ndi Mulungu.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 237 Munasiyatu
  • Hymn 1023 Kodi m’njiramo ndimvadi
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 104 M’mene ntchito yathatu,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 340 Imvani,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 1431 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 144 AMENE adzavomereza ndithu,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 200 YESU mundimve, ndikuliratu,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 1395 Mulungu ali nane!
  • Hymn 310 MBUYE munditsogolere,
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1717 Mtima wangawe, uyenera
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1020 Ngati umtsata Mpulumutsi wakoyo,
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 638 Ndi Mzimutu Woyera
  • Hymn 522 Akazi anadza
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1320 Ndayang’anira Mbuyeyo,
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 111 Nkhope yake ‘kabisika,
  • Hymn 436 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 108 MBUYE wondipulumutsa,
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 168 NDINGANENE malilime,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version