Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,
Next: Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1454 Ambuye, musendeze
  • Hymn 415 PAMAYIKO pali mdima,
  • Hymn 375 YESU m’khale nafe
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 1719 Ku Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1589 Ndinasokera kalelo,
  • Hymn 301 MBUYE, ndapangana
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1114 Akukumbukira
  • Hymn 332 Perekani mtima wanu,
  • Hymn 407 ADZAPAMBANA Yesu ponse
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 527 Idzani mumtima mwanga,
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 750 Yesu Mbuyathu, Inu nomwe ‘Nu,
  • Hymn 1691 Lero Kristu anauka, Aleluya,
  • Hymn 451 Yesu ndi Mbuyako,
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 27 “Msanga ndidzabweratu,
  • Hymn 356 YESU Mbuye onani,
  • Hymn 74 IDZA wolema,
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 1294 Wakuba uja nachiona,
  • Hymn 973 Tigwire nkhondo yomwe
  • Hymn 174 Haya, anzathu, itilinda nkhondo;
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 1567 Mubwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version