Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

  1. Home   »  
  2. Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda

 

TIIMBE nyimbo zotamanda
Mulungu wathu wabwino,
Pakuti akondana nawo
Anthu okhala padziko;
Tero natuma Mwana wake,
Wakukondedwa kalelo,
Kutiphunzitsa ife tonse
Za chikondano chakecho.

Mulungu ndiye wachifundo,
Nadzalandira onsewa
Akuulula mphulupulu
Ndi kukondana ndi Yesu
Tilondelonde njira yake
Yopapatiza yaing’ono;
Adzatilondolera ndiye
Kutifikitsa m’Mwambamo.

Pakuwoloka mtsinje wa imfa
Dzanja Mbuyathu agwira;
Tikadagwira ntchito zake
Atipatsatu korona;
Komwe kulibe masauko,
Pena misozi maliro;
Mulungu tidzamtamandira,
Inde kosalekezanso.

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 193 A! Kumwamba
  • Hymn 1198 Mabala ake m’manja
  • Hymn 1256 Chitsime ndi chokoma
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1624 Koma anthu onse omwe
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 136 Atumwi atummika, atumika,
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 248 Pena pakufadi,
  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 951 Ndi kale lonse mnandisunga ‘ne;
  • Hymn 717 Ambuye zathu zonsezi
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1032 Ntchito za Yesu gwira
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 89 Muli mphamvu yodabwitsatu
  • Hymn 361 AMBUYE munapatsa tsiku
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 361 Munka kangati kulawa
  • Hymn 421 Ine ndine mlendo
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 465 Yesu atiuza tiwale pa
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 112 Pangano lake m’mwaziwo
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1611 Nadzuka m’mandamo
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1655 Mbuye Yesu,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 1210 Kumwamba ndidzanenadi
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version