Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

 

KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Pochimwa anthu onsewo
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo
Wathetsa tchimoli.

Thupi la mwazi wathu ’li
Lochimwa kalelo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Laposa monsemo.

Choposa nalo thupilo
Chikhale momwemu,
Chiyeretsetsa m’katimo,
Ndi Mulungu Iyeyu.

Anatikondakonda ’Ye,
Ndi Mlungu Iyeyo,
Anatifera anthu ’fe
Ndi Mulungu Iyenso.

Ndi m’munda muja chete, phee!
Pamtanda pati njo!
Anaphunzitsa’bale ’fe
Titero ifenso.

Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 22 MU ZONSE abale yamikani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 1041 Zosauka unvomere,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 208 CHITHA n’chiyani kund’yeretsa?
  • Hymn 872 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 974 Tsopano timenyana
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1843 Chigwa choopsacho cha imfa ndikachilowera,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 1799 Mulungu atipatsa mphamvu
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 713 Ambuye, Mwini zonsezi,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 672 Mbwere Yesu Mwini moyo,
  • Hymn 882 Kodi tikulema nazo
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 470 Mutiletse tisaname
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 1402 Mverani Iye ati: idzanitu;
  • Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 113 Likalira llipengalo,
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1214 Mwamva Mzimu wakewo,
  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 355 Tinafuna m’phirimo,
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 163 MALO anachepa,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version