Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

  1. Home   »  
  2. Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

 

KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Pochimwa anthu onsewo
Nja Mlungu nzeruyi;
Adamu wachiŵiriyo
Wathetsa tchimoli.

Thupi la mwazi wathu ’li
Lochimwa kalelo,
Labweranso ku nkhondoyi,
Laposa monsemo.

Choposa nalo thupilo
Chikhale momwemu,
Chiyeretsetsa m’katimo,
Ndi Mulungu Iyeyu.

Anatikondakonda ’Ye,
Ndi Mlungu Iyeyo,
Anatifera anthu ’fe
Ndi Mulungu Iyenso.

Ndi m’munda muja chete, phee!
Pamtanda pati njo!
Anaphunzitsa’bale ’fe
Titero ifenso.

Kuuzani Mlungu m’Mwambamo
Mtamande m’kuyanso;
Nzozizwa nkhani zakezo,
Njolimba ntchito njo!

Post navigation

Previous: Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
Next: Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 693 Adzapambana Yesu ponse
  • Hymn 282 Ine ndili munthu
  • Hymn 438 TIYAMIKE Ambuye,
  • Hymn 390 A! YESU, ndapangana
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 213 Mawu a Yesu ati: “Msangatu
  • Hymn 10 Kristu Mfumuyo yaulemerero!
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 589 Koma ineyu
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 359 TADZUKA mzimu wanga ‘we,
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hello world!
  • Hymn 375 Zipatso zakezi
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 479 Munanena mulandira
  • Hymn 1616 Anafera
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1647 Kubweza inetu, kubweza inetu,
  • Hymn 1702 Pakufa ine Mbuye
  • Hymn 992 Mukandipweteka,
  • Hymn 258 Kazembe wanga m’matenda,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 665 Pomangidwa anthu nayo
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1777 Mulungu wamkulu
  • Hymn 963 Aulendo, munka kuti
  • Hymn 1355 Atate, Mwana, Mzimunso,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 463 MNANDIDZERA, Ambuye,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 284 Yesu Mfumu Inu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version