Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 181 PANALITU wakudwala

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1832 Za m’mdima, imfa, nkhondo ndi zoipa sindiopa;
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1348 Akupeza, akupeza,
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 183 MUDZE kwa Yesu, musachedwe.
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1000 Amatininkha zida zoteteza mtima, ndizo:
  • Hymn 38 Kodi mubvutidwa naye katundu?
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 1673 Lambira Yesuyo
  • Hymn 270 NDILIRA mtima wotamanda
  • Hymn 1278 Kuti muyeretsa mtima ndibvomeratu;
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 411 TAMVA mawu omwewo,
  • Hymn 1055 E, mtima watsopano ndi
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1289 Ndinasokeratu kutaliko,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 162 Angelo anu asunga
  • Hymn 456 Tizikondana, tisekere
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1766 Ndilikulemekeza
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 637 Mbuyathu wokondedwa,
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 1161 Wapumitsa mtima wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version