Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

  1. Home   »  
  2. Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 161 LERO lino mbale wanga,

 

LERO lino mbale wanga,
Ndilo tsiku lakukoma;
Talandira Mpulumutsi,
Mmene ali kuyitana.

Lero lino mbale wanga,
Usazengereze ayi;
Ngati ulandira Yesu,
Lero, udzachita mwayi.

Lero lino ndi labwino,
Moyo wako uli nawo;
Pena mawa umwalira,
Udzatani mlandu wako?

Lero lino mbale wanga,
Lapa mtima, lapa tchimo;
Yesu adzakulandira,
Ukam’pempha lero lino.

Ndiwe mlendo lero lino,
Myera ndikupempha iwe:
Yesu Mwana wa Mulungu,
Akufuna ndithu iwe.

Inde, lero lino Yesu,
Ayitana inu nonse;
Landirani Mpulumutsi,
Musazengereze konse.

Post navigation

Previous: Hymn 160 MADALITSO ngati mvumbi,
Next: Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 766 Monga zomera zonsezo
  • Hymn 63 Ndili nawo moyo w’satha
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 204 Kumandako, kumanda
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 313 Muthire, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 30 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 26 “Ndakukonda ku imfa
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 851 E, nthawi ya mamawayi
  • Hymn 876 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 560 Kale m’mzinda wachifumu
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 1478 Azizwa anthu ajawo,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 994 Limba mtima mbale wanga,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1540 Pankhope pathu mthirepo
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 582 A! Mulungu,
  • Hymn 311 Tifuna kuchita chifuniro chanu,
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 246 Pajapo ndipenya
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 268 POKHALA mtendere mu mtimangamu,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 442 Posachedwa tilekana
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,
  • Hymn 236 NDIDZIWITSITSA
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 685 Tamva mawu amwewo
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1117 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 255 Pakuona imfayo
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 1812 Kuzani Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 891 Akakusowa malo
  • Hymn 1178 Mawu omwewo, nyimbo yomweyi,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version