Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

 

ANTHU m’maiko onse
Akhala mitundu;
Kapena m’dziko lino
Akhala anzathu;
Agona mwa zoipa,
Apulukiradi,

Ati, Mutilangize
Abale, bwerani.

Ngakhale alemera
Ndi chuma cha dziko,
Kodi akakondwera
Opanda Mulungu?
Kodi akhala mwaŵi
Otsata zawozo?
Iyai, awonongeka,
Apeza tsokalo.

Ndi ife akudziŵa
Chikondi cha Mlungu,
Kodi tidzaŵamana
Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
Tichibukitsetu,
Kuti mitundu yonse
Ibwere kwa Yesu.

Akristu nyamulani
Maneno a Mulunguyo,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse;
Ndi Mwana wa Mlungu.

Post navigation

Previous: Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
Next: Hymn 129 WODALA ndiye munthuyo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 1298 Ndikhulupira ‘Nu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 843 M’maiko monse, zisi zomwe,
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 197 NDIKHULUPIRA’Nu,
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 222 NDILIKUMVA m’mtima mwanga
  • Hymn 906 Mulibe zoipa m’Dzikolo,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 814 Mutichiritse ifenso
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 738 Mommuno, Mbuye, mkate wanuwu,
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 961 Mbuye anatiitana
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 384 Mulungu akhale nawo
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 1028 Yendani bwino m’njiramo
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 1341 Tadza kukudyaku,
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 525 Afike masiku
  • Hymn 494 YESU Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 378 Ku madzi ake odikha
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
  • Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 957 Mundimwetse madzi anu,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 1551 Mukhale m’kati mwathu,
  • Hymn 895 Ndikabwera ndi katundu
  • Hymn 1657 Mbuye, mutsaganebe

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version