Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

  1. Home   »  
  2. Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 128 ANTHU m’maiko onse

 

ANTHU m’maiko onse
Akhala mitundu;
Kapena m’dziko lino
Akhala anzathu;
Agona mwa zoipa,
Apulukiradi,

Ati, Mutilangize
Abale, bwerani.

Ngakhale alemera
Ndi chuma cha dziko,
Kodi akakondwera
Opanda Mulungu?
Kodi akhala mwaŵi
Otsata zawozo?
Iyai, awonongeka,
Apeza tsokalo.

Ndi ife akudziŵa
Chikondi cha Mlungu,
Kodi tidzaŵamana
Kuŵala kwa Kristu?
Chipulumutso! Inde,
Tichibukitsetu,
Kuti mitundu yonse
Ibwere kwa Yesu.

Akristu nyamulani
Maneno a Mulunguyo,
Ndi moyo lalikani
Pa dziko lonselo;
Ndi Yesu Mpulumutsi
Anatiferatu;
Adzabvomera onse;
Ndi Mwana wa Mlungu.

Post navigation

Previous: Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
Next: Hymn 141 TAONANI pamtandapo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 79 PAKWITANA Mbuye wanga
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 898 Mndidziwitse ntchito yanga,
  • Hymn 968 Mzimu wakuipa
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1591 Sizitha ntchito zangazo,
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 68 M’MANDA, nagonamo
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 276 MKRISTU, ulimbike
  • Hymn 1061 Mundichotsere tchimo lonse
  • Hymn 306 Ona Mwanawanakhosayo
  • Hymn 1487 Bvumbulutsa zonse zako
  • Hymn 651 Ikhale ngati nyali
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1850 Anthu a mitundu yonse,
  • Hymn 95 TAMANI mphamvu ya Yesu,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 409 Yesu adza kuwerenga
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1441 Wochimwa iwe, bweratu
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 440 ZIKOMO Ambuye wathu,
  • Hymn 1331 Yesu wathu Mbuyeyo
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
  • Hymn 358 Dzina lake Yesuyo,
  • Hymn 464 Yesu atiuza tiyambemo,
  • Hymn 114 Ndine Mbusayo wabwino,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 1692 Timwimbire zomtamanda, Aleluya
  • Hymn 937 Chitsime chachikondi
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version