Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 105 IDZANI, Mzimu Inu,

 

IDZANI, Mzimu Inu,
Mundidalitse kuno;
Ndafoka mtima ine
Paulendo wanga uno;
Kwambiri ndakhumudwa
Panjirayo ya moyo;
M’kaleka kutsogola
Ndiwonongeka pompo.

Wakunga mwana ine,
Sindidziŵitsa konse;
Mundilangize Mzimu
Panjira yanga yonse;
Mundiyendetse bwino
Ndifike ine ndemwe
Panjira yolungama,
Kudziko la chimwemwe.

Mundilimbitse m’mtima
Pogwira ntchito izi;
Ndikapumula pena
Mukhale ndithu ndine;
Zolingirira zanga
Ziyere zonse m’mtima
Zoipa muzichotse,
Sindidzazichitanso

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1255 Chitha nchiani kund’yeretsa?
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 349 MOSE anamenya thanthwe kawiri,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 92 KONDA dzinalo la Yesu,
  • Hymn 451 MLUNGU alinane;
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 192 ZAKEYU mkulu wa misonkho,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 81 Imva mawu akewo,
  • Hymn 184 LEKANI kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1728 Zofuna zanga zonsezo
  • Hymn 386 MONGATU mawu anuwo,
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 640 Anakwatira kale
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 776 Tikondwereratu
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 954 Mbuye andipeza lero,
  • Hymn 475 MZINDA woyerawo
  • Hymn 947 Akristu tonsefe, tikondwe m’Dzikoli
  • Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 461 ANA inu, myamikeni
  • Hymn 476 Mpaka ndabvala mbuu!
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 746 Imfa ndi mdima zinathawa zii!
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 571 Kwa ife lero anabadwa
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1123 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 625 Chaka chino mutipatse
  • Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu
  • Hymn 1368 Mitambo inu yakumwambako,
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 1625 Ife tonse tikumbuke
  • Hymn 21 Mbuye mtsitsimutse!
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 41 Tiyeni, tiyeni,
  • Hymn 837 Koma kalelo mnakhalitsa pano,
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 49 ONA Mwanawankhosayo
  • Hymn 801 Lero mwatipatsa moyo,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 1720 Padzanja lachifundolo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version