Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

  1. Home   »  
  2. Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;

 

ATATE, tifika pamaso panu;
Mukomane ndi ife, Mbuye wathu.

Mitima yathu iyi nayo njanu,
Muiyeretse, muikonze Mbuye.

Ndi maso athu awa nawo nganu,
Muŵapenyetse zinthu zanu zokha.

Ndi manja athu awa nawo nganu,
Agwiretu ntchito yanu yokhayo.

Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
Ithamange m’ntchito yanu yokhayo.

Ndi milomo yathu iyinso njanu,
Ilalike Mawu anu kwa onse.

Ndi makutu athu awanso nganu,
Muŵamvetse Mawu anu okhawo.

Tidziperekadi konse kwa Inu
Tikakhale anthu anu okhawo.

Post navigation

Previous: Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
Next: Hymn 355 DZIKO lonse mlambire

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 143 KONZA mtima iwe mbale,
  • Hymn 958 Ndikalowa m’mtsinje muja,
  • Hymn 1836 Ndi wamwayi munthu uja
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;
  • Hymn 513 Atipempherera
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 245 KHALANI duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1520 Mbuye, Mawu anu
  • Hymn 310 Tafika kwa inu mutiunikire,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 502 Ndikonda mbiri yomwe
  • Hymn 75 Ndiperekatu
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 194 AMBUYE’naitan’ne;
  • Hymn 1208 Kalelo! Kalelo!
  • Hymn 1211 Mwakhulupiriradi
  • Hymn 1182 Chikhulupiro chomwenso
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 1015 Mbuye, mwatiuza ‘fe
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 439 MLUNGU wathu mwatifitsa
  • Hymn 1365 Zozizwa za m’dziko,
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1 NDINU wakuyera! Wamphamvu zonse.
  • Hymn 1220 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 559 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1128 Mbuyanga Yesu, mundisunge ine
  • Hymn 1816 Anatikondakonda ‘Ye,
  • Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 1529 Mndithandize kukondana
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 149 Ndisauka, sindikhoza
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 294 POYESEDWA ine
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 590 Mbuye, Msungi ‘Nu,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 207 Malo alimo m’nyumba ya Yesu,
  • Hymn 607 Dziko lonse lilikukondwa, mlengalenga mpheponso,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1497 Simbani mobwereza,
  • Hymn 460 KULI kaphiri m’talimo

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version