Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,

 

TIYENI, Akristu inu,
Mumenyane nkhondo iyi,
Mukafoka nonse, koma
Yesu akulimbitsani.

Muyendanso kunka komwe,
Mugonjetse mdani wanu;
Musafoke, musaleme,
Musagone konse inu.

Musagonje, anthu inu,
Mtamiretu Yekha Mbuye;
Ipambana mphamvu yake,
Ya Mtsogoli wanu yemwe.

Mtima wanu wonse ndithu
Udzakhala ndi chimwemwe.
Zida zanu mbvale bwino
Zakudzera m’Mwamba momwe.

Limbikani inu nonse,
Msangalalo ngwanu nokha;
Musaope kanthu kena
Mumtamire Mbuye Yekha.

Tiyeni ku nkhondo iyi,
Mugonjetse zonse konko;
Muingitse mdani uja,
Muyendetse m’njira momwemo.

Post navigation

Previous: Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
Next: Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 1200 Ambuye, m’imfamo
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 265 Imbirira moyo wanga,
  • Hymn 1095 Mumtima wakufatsa
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 516 Zitsamba zakuyera
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
  • Hymn 1310 Yesu wondikondadi,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 196 Tidzimba komweko nyimbo
  • Hymn 1465 Akulu inu m’bwere nonse,
  • Hymn 1572 Mumbveke, mbveke, mbveke,
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 385 SINDILI woyenera ’ne,
  • Hymn 1074 Mubweretu nomwe ‘Nu munatsika kalelo;
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 1637 Tisaleke kugwirabe
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 918 Ntchito yonse yakeyo
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 252 M’dziko lino chimwemwecho
  • Hymn 94 Ndani anatiwombola?
  • Hymn 1304 Ndi ine sizitheka ‘yi
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 1185 Imfa ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 535 Mbuye timlemekeze,
  • Hymn 822 Dzuwa lapitira,
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1035 Mphamvu zathu zonse
  • Hymn 468 NDIKONDWA kuti
  • Hymn 1703 Zathedwa zonsetu
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 62 AMBUYE Yesu,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 919 ‘Tate, mwa kusunga kwanu
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version