Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

  1. Home   »  
  2. Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 297 POKUMANA m’mayesero a dziko lino,

 

POKUMANA m’mayesero a dziko lino,
Matenda, imfa ndi usiwa;
Moyo umalefuka,
Ndikugwetsedwa mphwayi;
Mpaka nditamuuza Yesuyo.

Um fotokozere Yesu vuto lako,
Um fotokozere Yesu zonsezo;
Um’fotokozere Yesu vuto lako;
Adzakuchitira chifundo.

Pokumana m’mayesero a dziko lino,
Ndinasokera kutaliko;
Yesu nandigwira dzanja,
Nanditsogolera;
Mmene ndinamuuza zonsezo.

Abale tisachedwe ndi za dziko lino,
Za dziko lino ndi zachabe;
Yesu akufuna tibwere kwa Iye lero,
Kuti timuuzetu zonsezo.

Post navigation

Previous: Hymn 296 TIYENI Akhristu,
Next: Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 507 Yesu ndimkonda, akondanso ine,
  • Hymn 500 Mbuye Yesu andisunga
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 632 Tsopano tipereka mapemphero athu ano,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1259 Ndikhulupirira bwino
  • Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
  • Hymn 371 AMBUYE, tasonkhana
  • Hymn 209 M’NDILANDIRE ine Mbuye
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 296 Mngelo anatumidwa
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 422 Kwathu nkopambana,
  • Hymn 762 “Ndi thupi lopatsidwali
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 675 Pamaiko pali mdima,
  • Hymn 503 Ndikondwa kuti Yesu
  • Hymn 557 Usikuwo woyerawo!
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1091 Mulamulire mtima, Yesu,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1231 Nlokoma dzinalo la Yesu, ndilo thanthwe langa,
  • Hymn 66 Chisomocho chachotsadi
  • Hymn 188 Ine ndili ndi manyazi
  • Hymn 1042 Zonse umazinyadira
  • Hymn 1556 Mzimu Woyera, mudzetu kwa ine,
  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 325 KODI uli ndi chisoni
  • Hymn 1523 Atisangalatsa,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 593 Yesu, munditsogoza
  • Hymn 1741 Yesu munalaswa m’mtima,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1628 Dziko lino linaona
  • Hymn 829 Titamadi ‘Tate,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 45 Malawi dziko lokongola,
  • Hymn 1466 Ambuye wathu Yesu
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 1137 Masiku ena pali mdima,
  • Hymn 1398 Nditama mphamvu yake
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 59 IMVANI uthenga,
  • Hymn 1014 Tingolira kaya,
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 216 NDISAUKA, ndinachimwa,
  • Hymn 453 Tiana ta Ambuye tili
  • Hymn 293 Tidziperekadi konse kwa Inu
  • Hymn 215 TATE ndili mwana wanu,
  • Hymn 966 Kodi inu, aulendo,
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1700 Ambuye Mwini moyo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version