Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 240 YESU ndiye Mbuye wanga,
Next: Hymn 261 M’NDIYANDIKITSE nanu Yesu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 253 YESU ndinutu wanga m’njira zonse,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 169 ’MVANI liu lomwe
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1687 Alonda onsewo
  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1118 Ndifuna Inu Yesu,
  • Hymn 1662 Msandipitire, Yesu,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 443 M’MAŴA tizifesa
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1049 Zoipa zangazi
  • Hymn 376 Adzadalitsa ‘fe
  • Hymn 37 YESU analikhanda
  • Hymn 1761 Amithenga anaimba
  • Hymn 460 E! ang’ono ndifetu,
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 318 Ambuye, muli nazo zambirizi,
  • Hymn 277 GWIRA zintchito zako,
  • Hymn 1829 Mulungu ndiye Mbusa wanga, sindisowa konse;
  • Hymn 1552 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1001 Mafumu atiuza tikaletse ukapolo,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 292 Ndi makutu athu awanso nganu,
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 734 Ndi mkate wanu, Yesu
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1274 Chisoni andichotsera Mbuyeyu,
  • Hymn 940 Ndamvatu kuti tifika komweko
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 484 YESU ndiye Mbusa,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 1599 Inde, ndifuna kumvatu
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 394 Titanka kwathu mkhale nafeko,
  • Hymn 530 Munaneneratu mawu a moyonso
  • Hymn 116 Nkhosa zanga zimandimva
  • Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo
  • Hymn 202 NDIKHULUPIRIRA, Yesu,
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 401 A MULUNGU,
  • Hymn 1634 Pakwitana Mbuye wanga

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version