Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
Next: Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1512 Cholimbitsa mtima ndi
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 1180 Ndine kapolo wa Mbuye wanga;
  • Hymn 220 Kalekale ndinathawa,
  • Hymn 1176 Sandinyenga, salephera;
  • Hymn 1224 Inde ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 487 INE ndine mlendo
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 174 YESU wathu Mbuyeyo
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 621 Wolenga ndi Yemweyo
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 555 Mkucha wake ndaniyo
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 1457 Ndidziwa kuti Yesu
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 321 PAKUONA imfayo
  • Hymn 1651 Kwa Mulungu m’Mwambamo
  • Hymn 943 Onse aliko takonda kalelo,
  • Hymn 371 Mulungu, anthu ‘fe
  • Hymn 1674 Lambira Yesuyo,
  • Hymn 484 Mutiletse, Mbuye,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 138 Kumva ulikumva, ulikumva,
  • Hymn 1638 Alinkudza wansoni Munthu
  • Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 300 Ona Mwanawankhosayo
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1822 Lawani chikondano chake;
  • Hymn 1800 Kalelo anthu onse
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 83 Mpulumutsi Wokondedwa,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 1790 Imfa ya anthu ake imkomera,
  • Hymn 336 Perekani mtima wanu
  • Hymn 192 Apita anzathu dzuwa lino Kosaoneka,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 130 PHWANDO la Belisazara,
  • Hymn 318 TINALI ambiri ife,
  • Hymn 486 Yesu, Yesu,
  • Hymn 1813 Pochimwa anthu onsewo
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 1261 Kale ndinakana Inu, Ndinathawatu;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version