Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 243 KONDWANI nonsenu,

 

KONDWANI nonsenu,
Mpulumutsi anadza;
Onani kukhola,
Kumtanda ndi manda

Mlemekeze, bukitsani,
Naferatu kale;
Kondwerani, mlemekeze
Akhaladi moyo.

Kondwani nonsenu,
Anakhetsatu mwazi,
Natiwombola nawo,
Tikhale ana ’ke.

Kondwani nonsenu,
Atikhululukira,
Wosachimwa nafera
Anthu ’fe oipa.

Kondwani nonsenu,
Mfumu yathu yakwera;
Kwa Atate Kumwamba
Atipempherera.

Kondwani nonsenu,
Adzabweranso Yesu,
Waulemu, wamphamvu,
Kuweruza dziko.

Post navigation

Previous: Hymn 242 NDIIMBA mumtima mokondwa,
Next: Hymn 244 TIMVE za anamwali khumi,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 67 PAMENEPO pokhala madzulo,
  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 167 Yendanitu, Wansembe wathu,
  • Hymn 1342 Tadza kumtsinjeku
  • Hymn 377 Yehova, Mbusa wangadi,
  • Hymn 6 Nanu akukuzani amithenga,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 213 INE ndili ndi manyazi
  • Hymn 203 Pamtandapo, pamtanda,
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 338 Imvani
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 955 Komwe ndi chimwemwe ine
  • Hymn 299 “Posunga nkhosa ife
  • Hymn 1349 Salephera, salephera,
  • Hymn 12 Kumva milandu yathu mudzabwera
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 373 NYUMBA ya Mulungu, ili pano,
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 504 Pakumyamika Iye
  • Hymn 405 POLENGA dzikoli
  • Hymn 1272 Muyambe ntchito yanuyi,
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 127 POLUMIDWA ndi njokazo,
  • Hymn 1308 Ndi ine, m’mtima Mwanu mbee!
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 13 PAPHIRI ndi padambo,
  • Hymn 157 INU nonse ovutidwa,
  • Hymn 219 Mtenderewo wosanyenga
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 186 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 1144 Khalani duu! Ambuye adzatu;
  • Hymn 1405 Ati: “Undiuze
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 483 Ndife akuchoka,
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 561 Uyu ‘natsikira kuno,
  • Hymn 980 Tiyeni ku nkhondo iyi,
  • Hymn 962 Inde Mbuye, tibweradi,
  • Hymn 1801 Nafuna kwaononga
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 629 Tinayenda muli mdima
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 702 Mbuye wathu mutipatsa
  • Hymn 1448 Yesu ndiye Bwenzi lanu,
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 285 DZIKO lino lapansi,
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 794 Ambuye, tasonkhana
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 445 Mlewe oipawo,
  • Hymn 351 CHIYEMBEKEZO changacho,
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version