Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

  1. Home   »  
  2. Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,

 

UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
Inde, moyo tsopanopanotu;
Wolakwira upenye kwa Yesu Mbuyeyo,
Kuwombola naferatu ‘we.

Ona! Ona! Onatu!
Kuli moyo kwa yense
Apenya Yesuyo,
Wakuferatu pamtandapo.

Anasenzapo bwanji uchimo wonsewo,
Ngati wanu pa Yesu sulipo?
Bwanji mwazi wakhetsa kutsuka ifetu,
Ngati uwu sutikwanako?

Zilepheradi zonse kugula moyowo,
Koma mwazi wa Yesu Mbuyeyo;
Khulupi’ra mwamphamvu ya
Mlungu wathuyi,
Kuyeretsa’we m’mtima’komo.

Anatheradi pa mtanda ntchito zonsezi,
Zowombola mizimu yathuyi;
Ndipo yense akadza
Mokondwakondwadi,
Moyo apeza kwa Yesuko.

Post navigation

Previous: Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
Next: Hymn 152 AMBUYE wathu Yesu

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 73 M’SANDIPITILIRE Yesu,
  • Hymn 58 Titasokera tinabwerera,
  • Hymn 1453 Mukana Iye bwanji,
  • Hymn 252 MTIMA wa Mbuyako,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1760 Amithenga a Mulungu
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 587 Mutitsuke,
  • Hymn 254 Adzanena kwa anthuwo
  • Hymn 48 IMFA ya Mwana wa Mulungu,
  • Hymn 247 Tsono poukanso
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1621 Yang’anani anthu onse,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 1254 Mukhululukire ine,
  • Hymn 1300 Poyenda m’mdima bii,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1519 M’Buku lakuyerali
  • Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,
  • Hymn 90 WINA atikonda ife,
  • Hymn 1730 Anapeputsidwako,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1479 Ndi Yesu yemwe kalelo
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 983 Nkhondo ya Satana
  • Hymn 457 KALE m’mzinda wachifumu
  • Hymn 357 TAMANDANI Mbuye,
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1658 Idza wolema,
  • Hymn 435 Yesu ndiye Mbusa,
  • Hymn 238 Mbuye Yesu, lowani m’mtima,
  • Hymn 381 MONGA zomera zonsezo
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 227 Kasupe ali wodzaza
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 1148 Ndiimba mumtima mokondwa
  • Hymn 258 MWA ine, moyo wanga ndi Yesu
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 481 USACHIMWE konse,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 599 Mlengi wathu Wakuyera,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 481 Yesu wa Kumwamba,
  • Hymn 662 Tisaleme pakuchita zabwinozi,
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1609 Idzani nose’nu
  • Hymn 774 Tibatizidweko,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 1084 “Khala mwa Ine,” munachotsa tsoka,
  • Hymn 1425 Apempha malo Ambuye;
  • Hymn 393 ZOPEREKA tiperekazi,
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
  • Hymn 643 Mukhale nawo, yesu,
  • Hymn 121 Imbira!
  • Hymn 682 Tsatani Mbuye Yesuyo ndi mtanda wakewo;

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version