Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 110 MZIMU ndi mtogoleri
Next: Hymn 112 ELISA mneneri,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 597 Mlungu ali nane
  • Hymn 391 MUNDIMVERE, Mbuye wanga
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 117 Atate wondipatsazo,
  • Hymn 50 Akhristu nyamulani
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 1681 Mphamvu za imfa ndi za Satana
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 175 A! MBUSA wathu amvatu
  • Hymn 697 Zolengedwa zonse zidze
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 428 MBUYE mtsitsimutse
  • Hymn 372 DZUŴA la Mulungu
  • Hymn 857 Mlungu amaunikira
  • Hymn 916 Akondwerera anthu
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 605 Chifukwa cha zokoma mtima zonse za ulerezo,
  • Hymn 798 M’nyumba yanu, Mlungu, ‘yi
  • Hymn 370 KWACHA lero kwati mbee,
  • Hymn 68 Kwathu ndidzaimba nyimbo
  • Hymn 1698 Chinkana dziko lonselo
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 251 NDIFUNA Yesuyo,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 1808 Kutuma wabwereza,
  • Hymn 147 MUSAŴALOLE mawuwo
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 187 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 173 Mema nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 1648 Uko Kumwambako Mbuyangayo
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 15 Mbuye, chifundo chanu chitigwere
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 967 Mbuye, ndapangana
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 101 MZIMU Woyera, mudze mumitima mwathumo,
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 634 Mtifungatire ndi mapiko paulendo pathu,
  • Hymn 206 YESU, mulikundipempha
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 303 Ona pamtanda Yesuyo
  • Hymn 116 MBUYE, Mawu anu
  • Hymn 360 Muli ndi ludzu, idzani
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1408 Kodi mwalandira Yesu?

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version