Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

  1. Home   »  
  2. Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 111 YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;

 

YAKOBO mwanatu wachinyengoyo;
Wanyenga bambo ake
Kuti, “Inetu ndinetu
Esau mwana wanu.”

Esau analira, “abambo
Inu, abambo anga,
Ndabwera nayo nyama,
Mulandire, mudye.”

Thupi ndi Esau, koma mawuwo,
Ngatitu a Yakobo;
“Bwera mwana wanga,
Bwera pafupi n’kusisite.”

Ndapezatu bwenzi latsopanolo,
Ndi Yesu Mpulumutsi;
Yemwe angathe, kuchotsa,
Machimo anga onse.

Machimo andizunza ine;
Mtima mwangamu inedi,
Ndifuna Inu Mbuye,
Mulowe m’mtima mwanga.

Post navigation

Previous: Hymn 100 MUBWERE Mzimu Wakuyera,
Next: Hymn 121 MULUNGU, anthu ’fe

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 1612 Adzadza indetu
  • Hymn 805 Madzulo ano mkhaletu
  • Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 304 POZUNZIDWA inu ponseponse
  • Hymn 1356 Lemekeza Mlungu ‘Tate,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1397 Okwawa pansi inu,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 1325 Maiwe! Thanthwe long’ambikatu,
  • Hymn 817 Tibvomereze,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 80 Utsegule mtimawo,
  • Hymn 84 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1771 Iye natsitsa kunsi
  • Hymn 1583 Dzina la Yesuyo
  • Hymn 93 YAMIKANI dzina la Yesu Khrisituyo,
  • Hymn 180 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 186 MVERANI mbiri yozizwitsa
  • Hymn 1654 Mbuye, mutsaganetu
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 689 Anapeza Mwana
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1659 Ndiye mtsamiro
  • Hymn 233 AMBUYE Mulungu,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 274 YESU and’itana,
  • Hymn 1697 Onani m’mutu, m’manjanso
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 166 Yendani, Munthu Wachisoni,
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 324 Walira Yesu pazobvutazo,
  • Hymn 1807 Chithawa m’talitali
  • Hymn 97 Maso ndi maso ndi Kristu,
  • Hymn 40 Padziko pano tikhalira
  • Hymn 601 Akaona masautso
  • Hymn 492 DZIKO lilipolo
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 380 ATATE, muwapenya
  • Hymn 86 IYE wokhulupilira Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version