Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

  1. Home   »  
  2. Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 78 ALINKUDZA wansoni Munthu,

 

ALINKUDZA wansoni Munthu,
Wakukhala Kumwamba;
Alinkudza m’ulemerero,
Ndi Mwamuna wa mtanda.

Aleluya, Aleluya,
Alinkudza kwa ife;
Ndi chimwemwe
Tidzamkomana,
Pakufika Ambuye.

Alinkudza Ambuye Yesu,
Wakuphedwa pa dziko;
Alinkudza kukhala Mfumu,
Yoweruza mayiko.

Pakufika asonkhanitsa,
Anthu ake oyera;
Adzafuna mitundu yonse,
Omwe Iye ‘nafera.

Post navigation

Previous: Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
Next: Hymn 81 MBUYE Yesu adzabwera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 1396 Ndi maso Ambuyathu
  • Hymn 126 DAVIDE kubusa kuja,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 132 MVERA mtima wanga ’we
  • Hymn 247 MULUNGU anditsogolera,
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 289 Ndi manja athu awa nawo nganu,
  • Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 1005 Mdani adza nazo mphamvu,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1774 Poti akumbukira
  • Hymn 431 AKAPANDA kumanga,
  • Hymn 1071 Kumwamba Yesu mthandize,
  • Hymn 465 ANA a Yerusalemu
  • Hymn 71 Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
  • Hymn 1811 Tipulumuka mommo,
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 242 M’mene mubwera
  • Hymn 411 Yesu adza kukundika
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,
  • Hymn 52 POTULUKA m’mudzimo
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 1216 Ndatsatatsatabe
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 2 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 833 Mundilimbitse ndikayese manda ngati mphasayi,
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 396 PETURO ’nafunsa Hananiya:
  • Hymn 397 Yesu Mbusa, mutimvere,
  • Hymn 212 NDI MISOZI, ndi chisoni,
  • Hymn 133 NSEMBE yake ya Kaini,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 782 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 815 Dzuwa lapita,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 282 INU muli mehere,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1059 Kalelo m’mtima ndinakondwa,
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 1729 Munthu Wazisoniyo
  • Hymn 408 Oipa tili tonsefe;
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 17 MULUNGU ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version