Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 413 Yesu ndiye Bwenzi lathu,
  • Hymn 223 ATI Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 1656 Inu mundibisadi
  • Hymn 403 NDIYIMBA ndi chimwemwe lero,
  • Hymn 1167 Mulungu wanga,
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 275 Mlungu akuyang’aniredi,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 800 Yesu munadzukanso
  • Hymn 103 MPUME pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 784 Mugwade pansi m’nyumbayo,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 1159 Mwalembedwa mukalata
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1164 Tikakhulupira
  • Hymn 365 DZUŴA lapita,
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 53 AMBUYE Yesu anamva chisoni,
  • Hymn 1738 “Senzani mtanda wanuwo.”
  • Hymn 747 Tadzanitu, okhulupiradi,
  • Hymn 78 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 482 Ndinu wakuyera,
  • Hymn 1225 Ndinachita mphulupulu,
  • Hymn 1011 M’mawa tizifesa
  • Hymn 1024 Anasauka Mbuyeyo,
  • Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 374 Pakuti Mfumuyo
  • Hymn 461 Inu nonse anzanga,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 228 Ataya zoipa,
  • Hymn 65 NLA Mlungu dzuŵali:
  • Hymn 466 Yesu, muli pa chimpando
  • Hymn 1052 Ndilira mtima wotamanda
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1667 Yesu wakukoma mtima,
  • Hymn 732 1 Ndinamva njala, Yesu,
  • Hymn 288 Ndi maso athu awa nawo nganu,
  • Hymn 467 Ife ana sitiopa,
  • Hymn 304 Imva kulira kwa Yesu
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 325 Walira Yesu wolimbitsayo,
  • Hymn 1217 Chisoni chonsecho
  • Hymn 841 Mukhale, mukhale,
  • Hymn 604 ‘Tate, Mwana, Mzimu, ndinu
  • Hymn 1670 Bwenzi ndiye wakufera,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 611 Tidzakhala naye nthawi zonse ndi kuimbako,
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 250 Lidze msanga dzuwa lanu
  • Hymn 323 >APITA anzathu dzuŵa lino
  • Hymn 1122 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version