Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

 

NDI Aleluya imbirani,
“Tate wathu wa Kumwamba,
Analenga zonse;
Chifundo chake chachikulu,
Nzeru, mphamvu ndi ufumu,
Tiyamike tonse.

Ndi Aleluya imbirani,
Yesu Khrisitu Mpulumutsi,
Anachoka kwawo;
Nakhala munthu pansi pano,
Nasawuka, natifera,
Natisiira mawu.

Ndi Aleluya imbirani,
Mzimu wake wakuyera,
Amakhala nafe:
Atilangiza za Mulungu,
Nayeretsanso mitima,
Ya Akhrisitu ife.

Mulungu wathu tiyamika,
“Tate, Mwana,
Mzimu yemwe,
Aleluya Inu;
Woyera Inu, ndi wamphamvu,
Muyenera anthu onse,
Agwadire Inu.

Post navigation

Previous: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Next: Hymn 8 MITAMBO inu yakumwambako

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 294 Yesu anali khanda
  • Hymn 1156 Imfa ndi manda sitiopa ‘yi,
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1560 Mthandizi ndinu, mndithangate ine
  • Hymn 363 Funani Mlungu tsopano,
  • Hymn 688 Anthu akum’mawa
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1532 Mubwere kuno Mzimu ‘Nu,
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 129 Mudze kwa Yesu, musachedwe,
  • Hymn 544 Zoopsya sitidziwapo
  • Hymn 466 OSANATU, osana,
  • Hymn 671 Mbwere Mlungu Mbuye wathu,
  • Hymn 134 INU ansembe ngakhale mufunsa,
  • Hymn 395 Usiku uno mutisungedi,
  • Hymn 1219 Bwenzi ndinamkomanayo
  • Hymn 124 Aliponso adani am’kati ndi akunja;
  • Hymn 102 Mzimu ndi mtsogoleri
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1022 Mbuye, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 420 FESANI mbewuzo,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1235 Yesu wathadi
  • Hymn 1162 Mumvetu abwenzi athu,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 1087 “Khala mwa Ine,” Mbuye, ndifunitsa;
  • Hymn 1762 Anamva abusa omwe
  • Hymn 1849 Nthawi zonse monga ‘Tate
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 273 Mlungu akuyang’aniredi
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 434 CHIKONDI cha Mulunguyo,
  • Hymn 1104 Mndisungire mtima wanga,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1113 Mtima wa Mbuyako
  • Hymn 1375 Ndi anamwali obvekedwa mbuu!
  • Hymn 1677 Zomkweza zili m’Mwamba,Aleluya
  • Hymn 409 ANTHU akum’maŵa
  • Hymn 1549 Mtitsutse titachimwa
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1291 Njobvuta njira ndimayendamo,
  • Hymn 1721 Mapazi ake namvatu
  • Hymn 354 ATATE, tifika pamaso panu;
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 1369 Paphiri paja papakulupo,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 200 Ndi tsopano tilindira
  • Hymn 1568 Kudzoza kwanu kutipatsa
  • Hymn 10 TSOPANO linoli,
  • Hymn 1036 Mtima wakufatsa
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version