Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

  1. Home   »  
  2. Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

 

LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Lemekeza Mulungu Mwana,
Lemekeza Mulungu Mzimu,
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu,
Lemekeza, lemekeza
Mulungu wathu yemweyo.

Mlemekeze, anakonda
Natitsuka m’mtima mwathu;
Anatiwombola ife
Tikakhale ndi chifumu.
Lemekeza, lemekeza
Yesu Mbuye Nsembeyo.

Lemekeza Mfumu yathu,
Mfumu ya mipingo yonse,
Ipambana anthu onse
Akumwamba ndi apansi.
Lemekeza, lemekeza
Mfumu ya mafumuyo

Post navigation

Previous: Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
Next: Hymn 7 NDI Aleluya imbirani,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 496 MBUYE dalitsani Afirika.
  • Hymn 162 PENYETSETSA Yesu,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 365 Monga m’Mwamba mupambana
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 490 YESU adza kuwerenga,
  • Hymn 155 UTHENGA wa Mulungu
  • Hymn 227 NDIM’KONDE Kristuyo,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 1025 Ndikamayenda m’mdimamo,
  • Hymn 726 Mundidzze ndi chikondi,
  • Hymn 253 Adzakhala pampandopo
  • Hymn 670 Isaleke ntchito yake
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 1604 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1370 Mphepo yay’kulu yakuombayo,
  • Hymn 1344 Yamba ulendowo
  • Hymn 498 AMBUYE, mtidalitsetu,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1544 Wakunga mwana ine,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 280 Tisonkhane tonsefe,
  • Hymn 586 Yesu Mfumu,
  • Hymn 511 Ntchito zake zatha,
  • Hymn 312 Atate, mupatse zomwe tapemphazi,
  • Hymn 353 ATATE Wamkulu ndi Wamphamvu zonse,
  • Hymn 231 AMBUYE, m’imfamo
  • Hymn 228 MWAKHULUPIRIRADI
  • Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!
  • Hymn 548 Kale anthu m’kholamo
  • Hymn 1079 Khalatu woyera,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 376 PAMTANDA Mbuye anafera,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 1046 Ndiyere mbuu! E, ndiyere mbuu!
  • Hymn 1070 Mthandize Mbuye, timvetu,
  • Hymn 888 Polowa ndi Inu
  • Hymn 1596 Anamnyoza pansi pano,
  • Hymn 900 Mutipatse leroli
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1444 Wamoyo ndiye Yesudi,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 677 Ponse padakhala mdima
  • Hymn 379 Anditsogolera m’njira
  • Hymn 1389 Tithawire kwa Mulungu,
  • Hymn 1257 Mtanda m’mtima ndiyang’na,
  • Hymn 1685 Nla Mlungu dzuwali;
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version