Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

  1. Home   »  
  2. Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

 

LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
Lemekeza Mulungu Mwana,
Lemekeza Mulungu Mzimu,
Mulungu Mmodzi ndi wamkulu,
Lemekeza, lemekeza
Mulungu wathu yemweyo.

Mlemekeze, anakonda
Natitsuka m’mtima mwathu;
Anatiwombola ife
Tikakhale ndi chifumu.
Lemekeza, lemekeza
Yesu Mbuye Nsembeyo.

Lemekeza Mfumu yathu,
Mfumu ya mipingo yonse,
Ipambana anthu onse
Akumwamba ndi apansi.
Lemekeza, lemekeza
Mfumu ya mafumuyo

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1755 Choti timtumikire
  • Hymn 55 UNAKHETSEDWA mwazi do!
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,
  • Hymn 890 Kumbuka ‘bale ako
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 942 Kaamba chisomo cha Mbuyathu
  • Hymn 736 Mndidyetse m’chipululu
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 177 ŴALIRA Yesu m’dziko linoli,
  • Hymn 868 Atate yemwe anatuma Mpulumutsi mmodzi
  • Hymn 949 Mundiwalire m’njira mwangamo,
  • Hymn 1435 Ndiwe mlendo lero lino,
  • Hymn 347 Mfumu iyi,
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 765 Chikondi chili m’chikhomu
  • Hymn 515 Kuphiri la ‘Zitona,
  • Hymn 1586 Mbuye Yesu timtamanda
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1847 Ife tonse, ife tonse,
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1264 Chifuniro change, Mbuye, Ndiperekachi;
  • Hymn 20 CHIKONDI cha Mulungu wathu,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1461 Sing’anga ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 1124 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 894 Mbuye, ndinu Mfumu yanga
  • Hymn 35 Zonse za m’dziko zidzatha,
  • Hymn 1545 Mundilimbitse m’mtima
  • Hymn 71 DZIKO lino lapansi, ndilibetu abwenzi,
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 241 Munadzera ndi Mawu a moyo
  • Hymn 708 Peturo ‘nafusa Hananiya:
  • Hymn 1115 M’munda wa Mbuyako
  • Hymn 1317 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 488 Ndikabwera, Mbuye
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 569 Tiimbe ndi kulalikira
  • Hymn 733 Ndimamva ludzu Yesu,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1627 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 471 YESU Mbuye ’Nu wofatsa
  • Hymn 1443 Ambuye Yesu anatsira
  • Hymn 316 Ndikhazikike inetu,
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 858 Anthu osawerengeka
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 780 Kwezani mitu yanuyo,
  • Hymn 87 IDZANI nonse ’nu
  • Hymn 426 MBUYE, Mpingo wanu usauka kwakukuludi;
  • Hymn 459 KALE anthu m’kholamo,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version