Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 56 KU Mzinda wakuyerawo
Next: Hymn 58 PAMTANDAPO Ambuyeyo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 290 Ndi miyendo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 156 OKOMA ndiwo mawu
  • Hymn 740 Tsopano nthawi yake phwandili,
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 332 NDIKONDWA kuganizirabe
  • Hymn 1319 Ambuye naitana ‘ne:
  • Hymn 13 Mtiwerengere m’Mwamba ndi oyera;
  • Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 123 MULI ndi ludzu, idzani
  • Hymn 1769 Ndiye amachitira
  • Hymn 393 Tilikuimba nyimbo yomweyi,
  • Hymn 44 Mlungu dalitsani Malawi,
  • Hymn 441 MBUYE, tikuthokozani,
  • Hymn 922 Onse akulapawo
  • Hymn 887 Pakupempherera
  • Hymn 1121 Ndifuna Yesuyo,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 1580 Akadakhalabe
  • Hymn 254 PAMENE ndisawuka,
  • Hymn 1043 Mbiri yake ubukitse,
  • Hymn 24 TITAME Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 109 MUTHIRE, Yesu, m’mtimanga
  • Hymn 369 Lowani m’nyumba mwakemu
  • Hymn 946 Ngakhale enawo aleke kwimbako,
  • Hymn 88 Yesu, dzina lakukonda,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 642 Mulunzanitse awa,
  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 1578 Onsewa ‘nachimwa
  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 47 Anthu m’maiko onse
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 874 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 758 Sindili woyenera ‘ne;
  • Hymn 1050 Ndafoka inetu,
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1150 Pamtanda Mbuyanga ‘nafera,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 243 KONDWANI nonsenu,
  • Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 139 MLUNGU anapatsa moyo,
  • Hymn 875 Mtidzutse, Mbuyetu,
  • Hymn 43 Ulendo wathu ukadzatha
  • Hymn 520 Tamva tikondane naye,
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 999 Amaliwongo ochuluka amalowa m’mtima
  • Hymn 1481 Timsankhe Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 970 Pena kumwa nawo,
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 909 Ife tikondwera, ife tikondwera,
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version