Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

  1. Home   »  
  2. Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 57 TIYENI, dzalireni nane,

 

TIYENI, dzalireni nane,
Tidze ku mtanda wa Ambuye,
Tionse tichitetu maliro;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Kodi misozi itisoŵa,
Poona anthu amanyoza?
Onani umo apirira;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Anena mawu m’mtanda momwe
Mawu ochepa achifundo,
Apempherera ’dani ake;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Mtima wangawe, uyenera
Kuduka ndi manyazi lero,
Zamlasa ndi zoipa zako;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Ona chikondi cha Mulungu,
Ona zoipazo za anthu,
Koma chakula ndi chikondi;
Wapachikidwa Ambuyathu.

Post navigation

Previous: Hymn 40 KAMWANA Yesu ’nabadwa,
Next: Hymn 61 A! MUTU wakuyera,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1773 Monga anapangana
  • Hymn 430 MLUNGU akuyang’aniredí,
  • Hymn 141 Yenda iwe, yenda,
  • Hymn 495 Wonga Inu ndikhaledi,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 229 Woba wakufa ‘napenya
  • Hymn 149 RUTE, Rute anaumilira,
  • Hymn 1492 Sakukanani Yesudi,
  • Hymn 789 Ndi lokoma m’Mwambamo,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 1668 Kumdziwitsa ndiko moyo,
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 161 Tibwera ndi tianato
  • Hymn 1410 Nthawi zonse mufunabe
  • Hymn 1506 Ndikamfunafuna Iye,
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 832 Zochimwa za usana uno mndikhululukire ‘ne;
  • Hymn 1488 Musawalole mawuwo
  • Hymn 1737 “Senzani mtanda wanuwu.”
  • Hymn 929 Chikondano sichifera;
  • Hymn 493 DZUŴA li
  • Hymn 719 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 390 Lalowa dzuwa, kwada bii!
  • Hymn 1421 Alongo ‘nu, alongo ‘nu,
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 1504 Kodi ali ndi chilemba
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1110 Mulungu wanga,
  • Hymn 344 ’TATE, ’Nu.
  • Hymn 649 Inde, tikuyamikani, Atate, leroli,
  • Hymn 1496 Mawu amveke bwino,
  • Hymn 1361 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 706 Tisaiwalire ‘bale
  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 18 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 1775 Oonadi mtima,
  • Hymn 1538 Mzimu Woyera, mudzetu
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 1313 Zindichulukirazi
  • Hymn 123 Koma mudzisungire chuma cha Kumwamba
  • Hymn 233 M’mene ndapenya mwazi wa
  • Hymn 106 Ife, tapulumukadi,
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 55 Ambiri tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1516 Pakudera nkhawa ‘ne,
  • Hymn 687 Bukitsani mawunso
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version