Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

 

ATATE wa Kumwambako,
Munawombola ife, ndi
Chikondi chanu chijacho;
Tiyamikira Inutu.

Ambuye Yesu Inutu,
Munabadwira anthu ’fe;
Munatifera tonse ’fe;
Tiyamikira Inutu.

Mzimu Woyera m’mtimamo
Tiyeretsedwe ndi Inutu;
Munatisunga bwinoli,
Tiyamikira Inutu.

Atate, Mwana, Mzimunso,
Ndinu Atatu, Mmodzitu
Ochimwa tikupemphani:
Mutikhululukire’fe

Post navigation

Previous: Hymn 1858 Ha! Chikondi cha Mulungu,
Next: Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 541 Ana inu, yamikani
  • Hymn 1846 Mtima wanga uyamike
  • Hymn 1171 Mulungu wanga
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 342 Ambiri,
  • Hymn 938 A! Yesu Bwenzi langa
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 319 NDIDZATANI ine,
  • Hymn 136 MKAZI wa ku Samariya,
  • Hymn 1303 Aa! Mulungu wanga,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 93 Mverani mbiri yozizwitsa
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 1229 Dzinalo la Yesu,
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 96 Kodi mudzampembedza Mbuye
  • Hymn 1237 Ine kanthu ndilibe
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 433 MULUNGU wa Kumwamba bwera kunoku
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 1302 Ndi inetu sinditha ‘yi
  • Hymn 70 Mbuye ndinu bwenzi langa ndithu,
  • Hymn 256 Ndilira, ndilira,
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 190 Nsiku zonse kwanja kwake
  • Hymn 354 Tinafunafunatu,
  • Hymn 59 Tinachoka munjira ya imfa,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 578 Falitsani mbiriyi,
  • Hymn 1778 Angelo kwezani
  • Hymn 473 YESU wa Kumwamba,
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 1134 Pansi pano ndili mlendo,
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1489 Idzanitu, idzanitu,
  • Hymn 1622 Anthu onse amlambire
  • Hymn 871 Tiphatikane tonsefe okonda Yesu Kristu;
  • Hymn 410 Ana ake angonga
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 656 Ndipumulire panupo,
  • Hymn 769 Ndi kutsukidwa m’mwazimo
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 1301 Moyo ukatha zi,
  • Hymn 1501 Inde, pakufa panga
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 944 Tiyeni nonsenu okonda Yesuyo,
  • Hymn 1096 Tifuna Inu, Mbuye,
  • Hymn 1404 “Undipatsetu
  • Hymn 960 Tilikupita kwathu kuja
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 179 TUMPHATUMPHA moyo wanga,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 85 Mtima wanga wabvutika,
  • Hymn 243 Mtima wanga udzakondwera,
  • Hymn 808 Atipsinjadi masoka,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version