Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

  1. Home   »  
  2. Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,

 

ATATE wa Kumwambako,
Munawombola ife, ndi
Chikondi chanu chijacho;
Tiyamikira Inutu.

Ambuye Yesu Inutu,
Munabadwira anthu ’fe;
Munatifera tonse ’fe;
Tiyamikira Inutu.

Mzimu Woyera m’mtimamo
Tiyeretsedwe ndi Inutu;
Munatisunga bwinoli,
Tiyamikira Inutu.

Atate, Mwana, Mzimunso,
Ndinu Atatu, Mmodzitu
Ochimwa tikupemphani:
Mutikhululukire’fe

Post navigation

Previous: Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
Next: Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 1233 Tsopano ndibukitsabe chikondi chanu chija
  • Hymn 1752 Napulumutsa tonse
  • Hymn 42 “SENZANI mtanda wanuwu,
  • Hymn 1665 Nkhope yanu ndifunitsa,
  • Hymn 113 KALERO anthu onse
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 137 Yesu Mpulumutsi, Mpulumutsi
  • Hymn 133 Yesu watidzera, watidzera,
  • Hymn 249 MBUYANGA Yesu, mundigwire
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 1600 E! dzina la Yesu,
  • Hymn 536 Ana inu, myamikeni
  • Hymn 189 MLENDO ali pakhomo,
  • Hymn 941 Ndi Mbuyeyo tikhalamo,
  • Hymn 1246 Ambuyanga, ndalephera,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 1629 Adzabwera, adzabwera;
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 335 Mtembenuke mtima wanu,
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1601 Zina za Yesu ndimvetu,
  • Hymn 1359 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 95 Palibe mmodzi akanatha
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 925 Kodi umadandaula:
  • Hymn 1275 Mtima ‘we siya ndi Yesu nsonizi,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 16 Chikhulupiriro chathu
  • Hymn 1440 Yesu alindira,
  • Hymn 1644 Popachikidwa pa Golgotapo
  • Hymn 368 MULUNGU wanga, Dzuŵatu
  • Hymn 658 Ndichitireni, Mbuye ‘ne,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 821 Aleluya!
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 34 Yesu Mbuyetu, mwafera
  • Hymn 618 ‘Dzani Mbuye msangatu,
  • Hymn 595 Mbuye, ndinu wamphamvu,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,
  • Hymn 458 USIKUWO, woyerawo!
  • Hymn 1385 Anatsogolera kale
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 1399 Yesu ponong’oneza, idzanitu;
  • Hymn 1160 Ndinakhala wakuipa,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1357 Mlemekeze, anakonda
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version