Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 481 USACHIMWE konse,

  1. Home   »  
  2. Hymn 481 USACHIMWE konse,

Hymn 481 USACHIMWE konse,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 481 USACHIMWE konse,

 

USACHIMWE konse,
Lekatu kukwiya;
Uli mwana wake,
Mwana wa Mbuyathu.

Yesu ndi wofatsa,
Yesu ndi woyera;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima

Mzimu wakuipa
Ukusuzumira,
Umakuyesera
Kuti ukachimwe.

Koma usalole
Mawu a Satana;
Bweza tchimo lake,
Chita zolungama.

Yesu ndi Mbuyako,
Mbuyeyo ngwabwino;
Ana ake omwe
Aziyera m’mtima.

Post navigation

Previous: Hymn 480 TIANA ife tingofoka,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 257 Ndinasiya amayi,
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1514 Dzinthu zakumundazo
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 364 Ali wokhululukira;
  • Hymn 704 Monga tilandira, Mbuye,
  • Hymn 51 PANTHAWI yakufa Ambuye,
  • Hymn 1561 Mzimu Woyera, n’dzipereka ndense,
  • Hymn 620 Mphatso zonse zathu
  • Hymn 1223 Ndidzaimba za Mulungu,
  • Hymn 791 Anthu opembedzawo
  • Hymn 159 YESU ndi wokonda,
  • Hymn 819 Lero tigone,
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 287 POKONDWA ndi poona vuto
  • Hymn 303 MEMA nkhondoyo, wadza mdaniyo,
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 4 INU Mulungu, tikuyamikani;
  • Hymn 1284 Kale ndinalira Inu,
  • Hymn 327 NTCHITO yonse yakeyo
  • Hymn 763 Ndiponso m’manja chikhocho
  • Hymn 359 Tonse timyamiketu,
  • Hymn 574 A! Yesu Mbuye wakuyera,
  • Hymn 847 Konse kuli mdima bii
  • Hymn 641 Awiri aimamu,
  • Hymn 585 Alanditsa,
  • Hymn 592 Kuti m’Mwambamo
  • Hymn 1205 Ndikonda chifukwa
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 1493 Mbiri yakalelomwe
  • Hymn 1322 Ntchito zanga zonsezo
  • Hymn 446 Yesu alandira
  • Hymn 1417 Atate ‘nu, atate ‘nu,
  • Hymn 1108 Khala chete mtima wanga,
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 224 Atero ndaniyo?
  • Hymn 16 MTIMA wanga lemekeza,
  • Hymn 1840 Ndiye M’busa wanga,
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 1129 Mbuyanga Yesu, ndikapanda Inu
  • Hymn 1119 Ndifuna Yesuyo
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 965 Mundiuze, aulendo,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 92 Ufuna kugwira ntchito yake?
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 210 Nyumba yodyera ilikudzaza;
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1420 Abale ‘nu, abale ‘nu,
  • Hymn 570 Ndikhulupirira Yesu
  • Hymn 387 MUDZE, anthuni, talaŵani ’nu
  • Hymn 1854 Tate msandipitirire,
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 576 Kondwerani nonsenu

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version