Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

  1. Home   »  
  2. Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

 

ANTHU akum’maŵa
Nanka msangako,
Nzeru ’nali nazo,
Nafatsansowo;
Nanka kuli Mwana
Anabadwayo;
Anatsogozedwa
Ndi nyenyeziyo.

Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Nagwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.

Mu ulemerero,
Yesu m’Mwambamo
Muli eni ake;
Anthu onsewo
Osadziŵa konse,
Akutalinso,
Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.

Akukhala kunja,
Osokeranso,
M’ŵaŵalire Mbuye,
Asagone’wo;
Amumdima omwe,
Olemedwanso,
Mtsogoleri wawo
Ndi nyenyeziyo.

Paulendo wathu
Tili pansipa,
Muŵalire tonse
Tili m’njiramo;
Mutitsogolere
Anthu tonsefe,
Mutifitse tonse
Ndi nyenyeziyo.

Post navigation

Previous: Hymn 408 ABALE nonse mulindiranji?
Next: Hymn 410 MAWU akewo anamveka ponse,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 852 Munkhani zako zonsetu
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
  • Hymn 370 Pakuti Mbuye Mlunguyo
  • Hymn 1196 E! chikondi ndithu,
  • Hymn 1372 Zam’madzi zonse zakuopsyazo,
  • Hymn 1623 Adzatenga anthu ake
  • Hymn 1429 Penyetsetsa Yesu
  • Hymn 1004 A! mizimu yakuipa
  • Hymn 911 Mokhala mokhamokha
  • Hymn 188 MPULUMUTSI Wokondedwa,
  • Hymn 654 Ndilimbikitse, Mbuye, nji!
  • Hymn 1008 Wakuchezacheza naye
  • Hymn 741 Chakudya ichi chidzapita du,
  • Hymn 1351 Aleluya, Aleluya,
  • Hymn 1680 Aleluya, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1147 Khalani duu! Pakufa ifetu,
  • Hymn 1135 Mulungu anditsogolera,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 811 Wopulumutsa mudzetu;
  • Hymn 1418 Khulupirani kuti mukalowe m’Mwambamo,
  • Hymn 624 Ndinu mwatithangatira
  • Hymn 182 YESU watidzera, watidzera,
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 1559 Wotsogolera, munditsogolere
  • Hymn 1158 Yesu ndiye Mbuye wanga,
  • Hymn 707 Dalitseni, Mbuye, zonse
  • Hymn 1358 Lemekeza Mfumu yathu,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 128 ANTHU m’maiko onse
  • Hymn 263 AMBUYE mundisunge
  • Hymn 18 POKHALA Inu
  • Hymn 205 KWA Inu Yesu ndilira,
  • Hymn 1240 Ndilikuva m’mtima mwanga
  • Hymn 676 Adze amitundu yonse,
  • Hymn 295 Kubadwa kwa Yesu
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 240 Nyama za m’thengo
  • Hymn 432 Ulendo ungoyamba
  • Hymn 1426 Wina panalibe
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 699 Inu wakudzatu
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 150 MIPINGO iyo idzatu,
  • Hymn 591 Yesu Mwanatu
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 454 TAONANI, m’kholamo,
  • Hymn 1360 Ndi Aleluya imbirani
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 264 KHALATU woyera, pempheratu m’tseri;
  • Hymn 382 Mwadzoza mutu wanga ndi
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1371 Mitengo yaitalitali ‘nu
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 199 NDINASOKERA kutali,
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 418 UDINDO wolalikira Uthenga,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version