Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

  1. Home   »  
  2. Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 409 ANTHU akum’maŵa

 

ANTHU akum’maŵa
Nanka msangako,
Nzeru ’nali nazo,
Nafatsansowo;
Nanka kuli Mwana
Anabadwayo;
Anatsogozedwa
Ndi nyenyeziyo.

Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Nagwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.

Mu ulemerero,
Yesu m’Mwambamo
Muli eni ake;
Anthu onsewo
Osadziŵa konse,
Akutalinso,
Akokedwe iwo
Ndi nyenyeziyo.

Akukhala kunja,
Osokeranso,
M’ŵaŵalire Mbuye,
Asagone’wo;
Amumdima omwe,
Olemedwanso,
Mtsogoleri wawo
Ndi nyenyeziyo.

Paulendo wathu
Tili pansipa,
Muŵalire tonse
Tili m’njiramo;
Mutitsogolere
Anthu tonsefe,
Mutifitse tonse
Ndi nyenyeziyo.

Post navigation

Previous: Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,
Next: Hymn 421 ANTHU ali m’mdima akuyitanitsa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1455 Uthenga wa Mulungu
  • Hymn 1780 Titame Mlungu Wakumwamba,
  • Hymn 118 PANALI munthu amene,
  • Hymn 203 NTHAWI yathadi bwerera mbale,
  • Hymn 1075 Ndikhazikike inetu, mumtima muli mwai,
  • Hymn 1714 Tiyeni, dzalireni nane,
  • Hymn 1269 Ndifoka ndi zoipazo,
  • Hymn 1635 Pakwitana Mbuye wanga,
  • Hymn 849 Tadzuka mzimu wanga’we
  • Hymn 269 Atate ‘nu, amayi ‘nu, nonsenu,
  • Hymn 1726 Linadetsedwa dzuwa bii!
  • Hymn 1503 Ndikamzindikira ninji
  • Hymn 433 Zoipa ndi zabwino
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 1541 Tionetseni tonsetu
  • Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,
  • Hymn 383 Zokoma ndi zakuyanja
  • Hymn 3 TIMYAMIKIRE Mlunguyo,
  • Hymn 547 Anatikondakonda ‘Ye.
  • Hymn 936 Ukatha moyo wanga
  • Hymn 250 MBUYANGA Yesu,
  • Hymn 120 Lekani kubvutika ndi zinthu za padziko,
  • Hymn 1438 Yesu akukonda,
  • Hymn 1723 Unakhetsedwa mwazi do!
  • Hymn 43 GETSEMANI, Getsemani,
  • Hymn 1613 A Mulungu
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 1841 Kumadzi kuli njiratu andiyendetsa bwino,
  • Hymn 1080 Ambuye mundisunge
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1688 Mulibe m’mandamu,
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 969 Akathira nsembe
  • Hymn 619 Tilimalima m’minda,
  • Hymn 291 Ndi milomo yathu iyinso njanu,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 414 INU bambo, inu mayi,
  • Hymn 835 Mukhale ndine, dzuwalo lalowa,
  • Hymn 799 Inu Mlungu kalelo
  • Hymn 842 Tipempha kuti Mpingo wanu
  • Hymn 1535 Lichepa dontho lokhali,
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 1437 Yesu ndi wokonda;
  • Hymn 1060 Mubwere, Mzimu wa mpumulo
  • Hymn 314 TIYENI nonsenu okonda YESUYO,
  • Hymn 298 IFE tazingidwa ndi zinthu zoopsa,
  • Hymn 1382 E, chifundo chake chonse
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 755 Pamene padzakhalapo
  • Hymn 1423 Oipa inu nonsetu,
  • Hymn 1449 Pena imfa idza mawa,
  • Hymn 1810 Kalelo Mbuye Yesu
  • Hymn 1510 Mtume tsopanoli
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 329 Yesu atonthoza mtima
  • Hymn 420 Mtima umabisala
  • Hymn 1758 Poti Mulungu wathu
  • Hymn 244 Ndidze pafupi pa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version