Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 405 POLENGA dzikoli

  1. Home   »  
  2. Hymn 405 POLENGA dzikoli

Hymn 405 POLENGA dzikoli

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 405 POLENGA dzikoli

 

POLENGA dzikoli
Pakumva Inudi,
Kwayeratu;
Mumve pempheroli,
Ndipo pamenepo
Palibe mawuwo,
Muŵaletu.

Inu wakudzatu
Kuŵachiritsadi
Anthendawo,
Kupatsa moyowo,
Kuona m’masomo,
Pa anthu onsewo
Muŵaletu.

Mzimu woonadi
Ndi wachikondicho,
Idzanitu;
Muunikirepo
Pali zamdimazo,
Pa dziko ponsepo
Muŵaletu.

Inu atatuwo,
Wodala Mlunguyo,
Timveretu;
Pa dziko ponsepo
Muchotse mdimawo,
Mutume Mawuwo,
Muŵaletu.

Post navigation

Previous: Hymn 404 YANG’ANA mtanda wa Yesu,
Next: Hymn 406 M’MENE umauka m’maŵa,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1518 Zonse mwazilembamo,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 333 Perekani, perekani
  • Hymn 1798 Mukondwe anthu a Mulungu,
  • Hymn 668 Achisoni, obvutidwa,
  • Hymn 25 “Akaleka amake
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 308 AULENDO, munka kuti
  • Hymn 441 Tamverani, aitana:
  • Hymn 292 NDIPULUMUTSENI Mbuye,
  • Hymn 499 TIKUTHA kupemphera,
  • Hymn 1037 Mapemphero athu
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1632 Ndi chiyembekezo ichi
  • Hymn 164 Yendani, Mfumu yamtendere
  • Hymn 104 MUBWERE Mzimu Inu
  • Hymn 91 Ufuna kuyera kopambana?
  • Hymn 636 Yehova Mlungu wathu,
  • Hymn 850 Pemphero, pemphero,
  • Hymn 1245 Ine ndidzakuonetsa
  • Hymn 1855 Yesu, msandipitirire
  • Hymn 1733 Adzabwera Iyenso
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
  • Hymn 824 Yesu mutipatse
  • Hymn 1763 Amithenga anaimba
  • Hymn 99 Tsopano ndimwona Iye
  • Hymn 764 “Chikho cha mwazi wangachi
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
  • Hymn 1641 Pakufika asonkhanitsa
  • Hymn 1693 Koma masauko ake Aleluya
  • Hymn 742 Tikadya phando zaka zonsezi,
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 1056 Mkhalidwe wanu mundipatse,
  • Hymn 5 ATATE wa Kumwambako,
  • Hymn 1044 Yesu sakusiya konse;
  • Hymn 1067 Ambuyathu, ndikhumba tsiku lija
  • Hymn 33 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1127 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja;
  • Hymn 350 MBUYE ndayima pano,
  • Hymn 1517 Lindionetsera ‘ne,
  • Hymn 1406 Kodi ukafuna
  • Hymn 1759 Powalitsira omwe
  • Hymn 1716 Anena mawu m’mtanda momwe,
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 1640 Alinkudza Ambuye Yesu
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 191 AMBIRI tikondwera mwa Yesu,
  • Hymn 1394 Paphiri ndi padambo
  • Hymn 1282 Ndilinkudza kwa Ambuye,
  • Hymn 767 Munali mwana, Yesu ‘Nu
  • Hymn 1500 Simbani Mbiri yomwe,
  • Hymn 1101 Ngati mtima sumakonda
  • Hymn 1524 Ndiwo alimbitsa
  • Hymn 694 Sadalekeza kuyamika

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version