Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

  1. Home   »  
  2. Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 362 MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,

 

MUKHALE ndine, dzuŵalo laloŵa,
Wagwa usiku, bwenzi lindisoŵa;
Ndilibe wina wakundithandiza,
Wamphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

Kamoyo kanga katha lero lino,
Zidzachokanso zinthuzo za dziko;
Zimasinthika zonse zooneka,
Simusi nthika, mkhale ndinutu.

Koma kalelo mnakhalitsa pano,
Mukhale ndine, msandichokerenso,
Sin’pempha kuti Mbuye mungotsotse,
Komatu mukhalitse ndinetu.

E, tsiku lonse Inu ndifunitsa;
Ndi mphamvu yanu yokha ndisungika;
Mukatsogola ndidzadikha m’mtima;
Usiku, msana, mkhale ndinetu.

Adani sindiopa mukalipo
Muletse tsoka ndi chisoni chino;
Ikadza imfa n’dzalimbika m’mtima;
M’moyo ndi m’imfa mkhale ndinetu.

Post navigation

Previous: Hymn 360 KRISTU wakuyeratu,
Next: Hymn 381 MONGA zomera zonsezo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 54 MUNTHU wazisoniyo,
  • Hymn 122 Musadziunjikire chuma cha padziko,
  • Hymn 1172 Adzabweranso
  • Hymn 664 Komwe asauka anthu
  • Hymn 931 Tikagwidwa ndi chisoni,
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 8 Nanu Atumwi akumveka aja,
  • Hymn 317 UKATHA moyo wanga
  • Hymn 302 NDIDZE pafupi pa
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 67 Chisomo chandisungadi
  • Hymn 1731 Ife tinachimwadi,
  • Hymn 881 Tili nazo zotiyesa,
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1141 Pakulekana ifetu
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 120 MUNDINYEMERE ’ne
  • Hymn 666 Walitsani nyali yanu
  • Hymn 261 Munafera pa mtanda
  • Hymn 905 Iwo asekera, iwo asekera,
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 1826 Amadyetsa Iye mbalame zam’mwamba,
  • Hymn 39 MUNASIYATU dziko lanulo,
  • Hymn 1646 M’busa wokoma ndi Mbuyangayo,
  • Hymn 1593 Wina atikonda ife,
  • Hymn 384 USIKU uja kalero,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 950 Sindidapempha kale Mbuye ‘yi,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 323 Tiwaliretu, tiwaliretu
  • Hymn 993 Pakumalizidwa
  • Hymn 1130 Mbuyanga Yesu, mundigwire dzanja
  • Hymn 626 Inde, ‘Tate, mtiyendetse
  • Hymn 449 Mzimu wakuipa
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 131 Lolani ana, mumve Mlungu,
  • Hymn 234 IMFA ndi mfumu ya mdimawo,
  • Hymn 1639 Aleluya, aleluya,
  • Hymn 1439 Iwetu afuna,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 402 M’mtima mwangamu mlowemo,
  • Hymn 754 Ndi mtanda uli m’maso mbuu,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 1136 Mulungu anditsogolera
  • Hymn 1206 Ndidzakukondani
  • Hymn 1401 Imvani mawu ake, idzanitu,
  • Hymn 1145 Khalani duu! Mulungu wanuyu
  • Hymn 141 TAONANI pamtandapo,
  • Hymn 30 YEHOVA, Mbusa wangadi,
  • Hymn 1671 Akhululukira iwe,
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 1072 Mudzaze Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1027 Tithawiranji ifetu?
  • Hymn 1539 Kudzoza kwa Kumwambako
  • Hymn 478 Ndife ana, mutikonda,
  • Hymn 1595 Ndani mwa abale athu
  • Hymn 1619 Adzabwera,
  • Hymn 845 Ufumu wanu, Mbuye Yesu,
  • Hymn 568 Taukani, taonani

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version