Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 320 NDIKONDA Mlungu pomva Mbuye wanga
Next: Hymn 341 PAKUPEMPHERATU

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1792 Mulungu ndiye wachifundo,
  • Hymn 1833 Podwala ine pobvutidwa Andisamalira;
  • Hymn 839 Adani sindiopa mukalipo;
  • Hymn 1090 Chitsime chakuyera ine
  • Hymn 1236 Mbuye ndimva leroli
  • Hymn 1820 Kwezani nane Ambuyathu,
  • Hymn 349 Aitana,
  • Hymn 1547 Mtisangalatse m’zonse,
  • Hymn 523 “Ndidzawalandira,
  • Hymn 1381 Ndi mitima yokondwera
  • Hymn 1065 Ngakhale Satana andizunza ‘ne,
  • Hymn 334 Tsugulani mtima wanu
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1575 Tifuna kuti komweko
  • Hymn 79 Mlendo ali pakhomo,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 218 Mbuye Yesu ndi Atate,
  • Hymn 580 Mwana wakuyera ‘Nu,
  • Hymn 554 Iye ndani pamtanda
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 235 Kumwamba ndikaimbanso
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 125 Aliponso mabvuto, ena ndi oipa;
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 901 Musatifikitsemo
  • Hymn 617 Nthawi yina Mbuyeyu
  • Hymn 1307 Ndi ine simufuna ‘yi
  • Hymn 538 Iye anachoka kwawo,
  • Hymn 567 M’nyumba zonse ponseponse
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 432 KRISTU ndiye Mwala wathu,
  • Hymn 518 Ana a Yerusalemu
  • Hymn 19 Mbuye mtsitsimutse
  • Hymn 479 ANYAMATA inutu,
  • Hymn 383 KASUPE ali wodzaza
  • Hymn 820 Ndife ananu,
  • Hymn 1676 Kondwerani dzuwa lino Aleluya,
  • Hymn 1323 M’manja mopanda kanthu,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 193 THANTHWE long’ambikatu,
  • Hymn 1848 Tiyamike Mlungu wathu
  • Hymn 1193 Tsopano Mulungu
  • Hymn 1695 Pokumbukira mtandawo
  • Hymn 343 Auke,
  • Hymn 315 Munagwa pa Atumwiwo;
  • Hymn 346 PEMPHERO ndiko kufuna,
  • Hymn 1238 M’mene ndifa inedi,
  • Hymn 449 MLENGI wathu Woyeranu,
  • Hymn 1295 Ambuye, mwazi wanuwo
  • Hymn 175 Mlungu mverani, mphamvu patseni,
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 139 Bwerani inu nonse, inu nonse,
  • Hymn 998 Anatilemba Yesu tikagwire nkhondo yake,
  • Hymn 1133 Ngatitu abwenzi anga
  • Hymn 1573 Inu osankhidwa ake,
  • Hymn 153 NDAKUMANA ndi bwenzi lokomalo,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 232 Uchita kwombola,
  • Hymn 208 “Lowa, lowa
  • Hymn 855 Aulendo amayenda

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version