Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

  1. Home   »  
  2. Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,

 

KWATHU sipadziko, ndingopitilira,
Ndadzikundikira chuma Kumwambako;
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye, ndi ‘Nu Bwenzi langa ndithu.
Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu?
Mngelo akodola pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,
Mpulumutsi wanga wandikhu’lukira;
Adzandipyoletsa pamene ndafoka,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mbuye watsogola ku Ulemerero,
Ndifuna kugwira dzanja lake konko;
Andidikiranso pakhomo la M’mwamba,
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.

Mu Ulemelero tidzakhala m’yaya,
Oyera mtimawo ali kulambira;
Ati: “Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,”
Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu

Post navigation

Previous: Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
Next: Hymn 336 KULINSO dziko lowala M’mwamba,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 413 ZIPATA zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 1446 Inu nonse obvutidwa,
  • Hymn 23 TIIMBE nyimbo zotamanda
  • Hymn 1378 Tsopano linoli
  • Hymn 334 KULI dziko labwino M’mwamba,
  • Hymn 1222 Bwenzi ndimamkomanayo
  • Hymn 566 Ana inu, ana inu,
  • Hymn 673 Mbwere Mzimu Wakuyera,
  • Hymn 885 Mndimvetse chisoni
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1432 Lero lino m’bale wanga,
  • Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
  • Hymn 290 NAMONDWE wawuka,
  • Hymn 358 MLUNGU ali muno,
  • Hymn 176 AITANA, aitana dziko lonse,
  • Hymn 232 WAFUNAFUNA ine
  • Hymn 265 MUDZAZE Yesu mtima wanga ndi chikondicho,
  • Hymn 1768 Ndiye wamphamvu zonse
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 884 Mndikumbutse zomwe
  • Hymn 279 MBUYE, nditsate bwanjiko?
  • Hymn 345 Ubwere,
  • Hymn 711 Ife tonse tichenjere
  • Hymn 1379 Mulungu yemweyo
  • Hymn 603 Mzimu wanu Wakuyera,
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 64 Mantha, nkhawa, ndi chisoni
  • Hymn 23 Mvera mtima wanga ‘we
  • Hymn 148 Ndisauka, ndimasowa
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye
  • Hymn 1834 Chisomo ndi zokoma zake sizileka konse;
  • Hymn 337 PADZIKO pano tikhalira M’moyo wosauka;
  • Hymn 145 Kale ndinafuna
  • Hymn 1414 Zonse zinathedwadi;
  • Hymn 485 Mukatiitana
  • Hymn 648 Mulungu wa Kumwamba,
  • Hymn 48 Ngakhale alemera
  • Hymn 82 Mlendo wa Kumwambayo
  • Hymn 1844 Pamaso pa adaniwo mwayala gome langa;
  • Hymn 727 Imfa ikandifikira,
  • Hymn 1188 Akumangidwa ndi mzimuwo,
  • Hymn 1678 Yesu nkana saoneka, Aleluya,
  • Hymn 234 Kwa kutha kwa moyo,
  • Hymn 1290 Ndilibe malo mokhaliramo,
  • Hymn 110 Ndaima nji pa Kristuyo,
  • Hymn 417 M’manja a Yesu wanga
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 199 Watitsogolera Mbuye,
  • Hymn 663 Anyamata a Mulungu,
  • Hymn 1068 Ambuye, thandizenitu
  • Hymn 1531 Kudzirala ndi kufatsa,
  • Hymn 859 Pakufika tsidya lija,
  • Hymn 447 Usachimwe konse,
  • Hymn 1142 Tidzathawira kuti ‘fe
  • Hymn 1393 Nditamatu Ambuyangayu,
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1498 Simbani Mbiri yonse
  • Hymn 1669 Ukafuna kumdziwitsa,
  • Hymn 448 CHIFUKWA cha zokoma mtima zonse zaulelezo,
  • Hymn 457 Palibe mwana wakuchepa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version