Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 300 AKRISTU limbikani,
Next: Hymn 321 PAKUONA imfayo

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 379 MTSINJE woyerawo
  • Hymn 41 MKATI mwa zovuta zathu
  • Hymn 438 Yesu ndiye Mbusa
  • Hymn 781 Tatsegukani inutu,
  • Hymn 153 Pemphero ndiko kufuna,
  • Hymn 1542 Titamire nthawi zonse
  • Hymn 1078 Khalatu woyera
  • Hymn 345 ATATE, ndipempha
  • Hymn 1311 Pothawira pena ‘yi,
  • Hymn 72 YESU wakukoma mtima,
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 598 Mlungu ali nane;
  • Hymn 26 NDIKULEMEKEZA
  • Hymn 1495 Simbani bwinobwino
  • Hymn 84 LIDZE msanga dzuŵa lanu
  • Hymn 107 Panalibe mwa abale
  • Hymn 512 ‘Natipulumutsa
  • Hymn 1508 Mundinyemere ‘ne
  • Hymn 588 Mlungu, Inutu,
  • Hymn 1387 Amaweta nyama zonse,
  • Hymn 296 TIYENI Akhristu,
  • Hymn 1010 Ndipo ngati ungolema,
  • Hymn 1557 M’phunzitsi, ndinu mudziwitse ine
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 1483 Pakupempha ife pano,
  • Hymn 308 Ifetu kuchimwa, Mbuye,
  • Hymn 1803 Nowayo nayendamo,
  • Hymn 1377 Ndi amithenga akumwambako,
  • Hymn 305 NDALIMVA dziko la m’talimo,
  • Hymn 395 AMBUYE, Mwini zonsezi,
  • Hymn 556 Ndani pachimpandocho
  • Hymn 331 Yesu ndimafuna Inu,
  • Hymn 1484 Idzatu, idzatu
  • Hymn 1034 Mkristu, ulimbike
  • Hymn 1838 Ndiye Mbuye wa ambuye;
  • Hymn 1329 M’tali mutali m’phirimo
  • Hymn 606 Dzinja lokondweretsa lafikanso,litapumatu,
  • Hymn 1509 Mkate wamoyowo
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 87 Aleluya, mwandigula,
  • Hymn 1462 Dzina la Yesu ndi lokoma,
  • Hymn 1093 Odala ndi onsewo
  • Hymn 450 Koma usalole
  • Hymn 1276 Ndikhulupirira, Yesu, Inu nokhadi
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 190 CHITETEZO chachikulu
  • Hymn 356 Tinafena m’nyanjamo,
  • Hymn 1138 Masiku onse m’mtima mwanga
  • Hymn 579 Pochezera m’dambomo,
  • Hymn 1345 Iwe tiye, iwe tiye,
  • Hymn 1754 Ndiye akumbukira
  • Hymn 549 Ndiye Mbuye, Mfumu yanga,
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 77 Ndipereka zanga zonse,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 402 BWERANITU, bweranitu,
  • Hymn 1475 Anathera pamtanda zintchito zonsezi
  • Hymn 1097 Njira yanga sindidziwa,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version