Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

  1. Home   »  
  2. Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 312 NDIMAYENDA paulendo

 

NDIMAYENDA paulendo
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhaŵa, mantha,
Amadziŵako.

Ichi chindisangalatsa
M’mene nkhondo indigwira,
M’mene nsoni zazikulu
Zimanditsatira;
Mtima ukhazika m’mene
Kwathu kuja ndikumbuka
Kuti Mlungu ali ndine,
Andisungako.

Mbuye andipeza lero,
Andikonda, andisunga;
Adzapitikitsa mdani
Akamandibvuta.
E, ulendo wanga utha,
Tsono ine ndimwalira;
M’mene ndidzafika kwawo
And’landirako.

Komwe ndi chimwemwe ine
N’dzaonana ndi Atate,
N’dzagwadira ndi kumtama,
Amandikondabe.
Sakandisautsa kanthu
M’dziko lija lakukoma;
Adzandidalitsa Yesu,
Ndidzakondwako.

Post navigation

Previous: Hymn 311 VALANI zida tizinka kwathuko,
Next: Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1186 Yesu anafa pamtandapo,
  • Hymn 6 LEMEKEZA Mulungu ’Tate,
  • Hymn 1823 Opani Iye, nimuleke
  • Hymn 1003 Kanganani nkhondo yanu
  • Hymn 207 AMBUYE ndamvatu Mawu anu,
  • Hymn 327 Yesu salephera ‘yi.
  • Hymn 1039 Usafune chuma chokha,
  • Hymn 338 ’TATE wa Kumwambako,
  • Hymn 205 Pakukwera Kumwamba
  • Hymn 1352 Atate wa Kumwambako,
  • Hymn 155 Pemphero ndiko kufuna
  • Hymn 61 A! MUTU wakuyera,
  • Hymn 788 Moyo watsopano
  • Hymn 646 Mudalitse nyumba yathu;
  • Hymn 1383 Dzina lake tibukitsa,
  • Hymn 1262 Lero mtima ungolema, Usaukadi;
  • Hymn 1672 Lambira Mfumuyo,
  • Hymn 364 DZUŴA lapitira,
  • Hymn 398 Lero lino mwatipatsa
  • Hymn 89 INDE, ndifuna kumvatu,
  • Hymn 181 PANALITU wakudwala
  • Hymn 679 Zipata zachitsulo zitseguke zonse mbee!
  • Hymn 429 M’DZANJA lanu Ambuye,
  • Hymn 288 HAYA! ’nzanga taonani
  • Hymn 27 LEMEKEZANI Yehova,
  • Hymn 80 KUDZA kwa Mbuye
  • Hymn 1679 Tiyamike Dzina lake, Aleluya,
  • Hymn 615 Yamikani nonse ‘nu,
  • Hymn 313 MUNDIŴALIRE m’njira mwangamo,
  • Hymn 1140 Paja athira Yesutu
  • Hymn 896 Mbuye, ndinalema ine,
  • Hymn 1125 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 1594 Chikondano chakechi
  • Hymn 1757 Udzadziwitsa anthu
  • Hymn 705 Tikhaletu nawo, Mbuye,
  • Hymn 721 Anu Mbuye ndifetu!
  • Hymn 185 NDINE Mbusayo wabwino,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 1748 Ambuye tsopano lino,
  • Hymn 1058 Chimwemwe chija chamumtima
  • Hymn 1324 M’moyo uno kunsiku
  • Hymn 1413 Ndichitenji kukapeza
  • Hymn 692 Paulendo wathu
  • Hymn 1430 Ndipo pakulowa
  • Hymn 107 MUBWERE kuno Mzimu ’Nu
  • Hymn 681 Ankhondo a Mulungu ‘nu, yendani m’njiramo,
  • Hymn 775 Mwa anthu onsewo
  • Hymn 1155 Abale angakhale m’talimo
  • Hymn 137 UTHENGA wa Ambuye
  • Hymn 1750 Ndi nyali yakuwalitsa
  • Hymn 748 Ndiye wa moyo wonse Mwiniyo,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 972 Akristu limbikani,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 177 Tate, ndili mwana wanu,
  • Hymn 1336 Mwamva mawu a Mulungu;
  • Hymn 165 ATATE,’nu, atate ’nu,
  • Hymn 216 Ndi misozi ndi chisoni
  • Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version