Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

 

AKRISTU limbikani,
Imani mtima nji!
Mbendera nyamulani,
Msatenthemere ’yi.
Wotsogolera wathu
Ndi Mwana wa Mulungu;
Adzagonjetsa onse
Adani athuwo.

Tigwire nkhondo yomwe
Ya Mbuye wathuyo;
Tileke zakuipa
Zokhala m’mtimamo.
Sitikwanira tokha
Kuleka zathu zomwe,
Koma Mbuyathu Yesu
Atithangatatu.

Tsopano timenyana
Ndi zakuipazi;
Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
Yesu adzalandira
Ankhondo ake onse;
Adzakhalika naye
Kumwamba komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 644 M’wasunge, m’wayendetse
  • Hymn 45 IFE timakufunani
  • Hymn 57 Ife tiyembekezera Yesu,
  • Hymn 1764 Yesu ndinu Mbuye wathu,
  • Hymn 1306 Ndi ine ndasaukadi,
  • Hymn 1515 Ndikachimwa, Bukuli
  • Hymn 285 Ndipempha, Ambuye,
  • Hymn 178 Machimo anga ngambiri
  • Hymn 70 LAMBIRA, Mfumuyo,
  • Hymn 399 M’KHOLA mwa ng’ombe ku Betlehemu
  • Hymn 1818 Kuzani Mlungu m’Mwambamo
  • Hymn 1459 Ambuye mulowetse
  • Hymn 415 Tidzalandirabe komwe
  • Hymn 1386 Ndi chifundo atipenya
  • Hymn 744 Kristu ndi mwini moyo wathuwu,
  • Hymn 827 Wonsewu usiku
  • Hymn 1660 Ndikakhumudwa
  • Hymn 1626 Mbuye Yesu adzabwera,
  • Hymn 480 TIANA ife tingofoka,
  • Hymn 1407 Tula mtolo wako
  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 339 Tipempha,
  • Hymn 315 YENDANI munjira yake,
  • Hymn 382 M’wabatize anzathuwa,
  • Hymn 439 Nthawi yaubwana yatha,
  • Hymn 1747 Yesu aitana ife;
  • Hymn 920 Yatha misoziyo,
  • Hymn 1139 Namondwe akawombabe,
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 450 YESU, munditsogoza
  • Hymn 31 MULUNGU Wamkulu,
  • Hymn 28 Mbuye ndisaukadi,
  • Hymn 473 Mzinda woyerawo!
  • Hymn 1422 Abwenzi ‘nu, abwenzi ‘nu,
  • Hymn 286 Atate, tifika pamaso panu;
  • Hymn 1151 Pomulambira Yesu Mbuyanga,
  • Hymn 392 Chimwemwe chomwe mpatseko
  • Hymn 15 YEHOVA ndiye Mbusa wanga,
  • Hymn 1266 E, chimwemwe chachikulu, N’taperekadi
  • Hymn 73 Mu ulemerero tidzakhala m’yaya,
  • Hymn 1856 Mzimu, msandipitirire,
  • Hymn 1132 Mlungu adzandilandila,
  • Hymn 3 Ndinu wakuyera!
  • Hymn 1179 N’kamvera Yesu ndikakondwera,
  • Hymn 259 CHISOMO chodabwitsacho,
  • Hymn 1285 Yesu, n’kupatsani zonse,
  • Hymn 1740 Yesu, ndi chifundo chanu
  • Hymn 483 NTHAŴI yaubwana yatha,
  • Hymn 1473 Anasenza pa bwanji uchimo wonsewo,
  • Hymn 602 Mpulumutsi wakukoma,
  • Hymn 1234 Ati Yesu Mbuyeyo:
  • Hymn 12 NDITAMATU Ambuyangayu,
  • Hymn 1191 Ambuyanga Yesu
  • Hymn 1631 Mudzabwera, mudzabwera;
  • Hymn 99 TIYAMIKE mbuye Yesu
  • Hymn 262 Tumphatumpha moyo wanga,
  • Hymn 50 PAUSIKU uja,
  • Hymn 135 USANABADWE, Yeremiya,
  • Hymn 182 Kondwani nonsenu,
  • Hymn 119 M’BUKU la moyotu Mbuye,

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version