Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

  1. Home   »  
  2. Hymn 300 AKRISTU limbikani,

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 300 AKRISTU limbikani,

 

AKRISTU limbikani,
Imani mtima nji!
Mbendera nyamulani,
Msatenthemere ’yi.
Wotsogolera wathu
Ndi Mwana wa Mulungu;
Adzagonjetsa onse
Adani athuwo.

Tigwire nkhondo yomwe
Ya Mbuye wathuyo;
Tileke zakuipa
Zokhala m’mtimamo.
Sitikwanira tokha
Kuleka zathu zomwe,
Koma Mbuyathu Yesu
Atithangatatu.

Tsopano timenyana
Ndi zakuipazi;
Pamene nkhondo yatha
Tidzanka kwathuko.
Yesu adzalandira
Ankhondo ake onse;
Adzakhalika naye
Kumwamba komweko.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1732 Anapachikidwatu,
  • Hymn 953 Ichi chindisangalatsa
  • Hymn 151 UKAPENYA kwa Yesu uliko moyoko,
  • Hymn 348 CHIKHULUPIRIRO chathu
  • Hymn 1239 Ndipo pakuima phe!
  • Hymn 855 Aulendo amayenda
  • Hymn 224 LINDIKOMERA dzina la Ambuye Yesu wanga,
  • Hymn 1795 A! chikondi chachikulu
  • Hymn 1739 Ife timakufunani
  • Hymn 1053 Mtimatu wopirira ndi
  • Hymn 914 Nlokoma Dziko langa!
  • Hymn 389 NDIMAMVA njala, Yesu,
  • Hymn 990 Poyesedwa ine
  • Hymn 1051 Zin’sowa indedi
  • Hymn 933 M’mene imfa yathu idza,
  • Hymn 459 Aphunzitse anthuwo,
  • Hymn 489 Yesu, ndikabwera,
  • Hymn 143 Lero lino Mbuye Yesu
  • Hymn 32 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 529 Zili nazotu nkhwimba zirombozo,
  • Hymn 154 SING’ANGA ‘mkulu ndiye Yesu,
  • Hymn 745 Anatifera nsembe Iyeyo,
  • Hymn 1554 Mpume pa inetu, Mpweya wa Mulungu,
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 1787 Mulungu wanga ndiye wachifundo
  • Hymn 1248 ‘Dzanitu Wamphamvu yonse,
  • Hymn 1173 Sindinanyengedwa konse
  • Hymn 1744 Kale ophunzira ake
  • Hymn 1584 Konda dzinalo la Yesu
  • Hymn 1614 Anabadwa,
  • Hymn 533 Ananu, ziimbani,
  • Hymn 752 Chakudya chakumwambachi
  • Hymn 1066 Uchimo unapachikidwa pomwe
  • Hymn 1227 Ndiyamika Mbuye wanga
  • Hymn 1243 Kodi mayi wobereka
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1166 Masauko athu
  • Hymn 305 M’mwazi wake tisambamo;
  • Hymn 501 Yesu andikonda ine;
  • Hymn 1463 Zoipa zakhululukidwa,
  • Hymn 1218 Pakufa pangapo
  • Hymn 214 KUNALI munthu ku Yeriko,
  • Hymn 172 TADZA kukudyaku,
  • Hymn 1315 Ambuye ‘naitana ‘ne:
  • Hymn 792 Dzuwa la Mulungu
  • Hymn 1537 Mulowe m’mtima, mdzazetu
  • Hymn 1018 Yesu afuna iwe unnke kwawoko,
  • Hymn 1743 M’kati mwa zobvuta zathu
  • Hymn 264 Bvinabvina moyo wanga,
  • Hymn 339 MTIMA wanga ndikonzera,
  • Hymn 176 Mleke mdaniyo, mwimbe m’njiramo
  • Hymn 462 ANANU, ziimbani,
  • Hymn 1126 Ndifuna Inu, Yesu,
  • Hymn 44 NTHAWIYO anam’gwira Yesu,
  • Hymn 201 NDILINKUDZA kwa Ambuye,
  • Hymn 1203 Zambiri zangazo
  • Hymn 66 >ALELUYA, Aleluya, Aleluya!
  • Hymn 1415 Iye anatsika m’Mwamba,
  • Hymn 1442 Khulupira mawu onse
  • Hymn 146 KODI ulikulemedwa

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version