Skip to content

Mon - Sat: 8.00 - 18.00

04463235323

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 280 YESU, afuna iwe unke kwawoko,
Next: Hymn 301 MBUYE, ndapangana

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 753 Getsemane ndionako
  • Hymn 531 Pakubweranso Inu m’Ufumuwo
  • Hymn 844 Pogona ife, amadzuka
  • Hymn 398 KODI mbale wasimba zachikhululukiro,
  • Hymn 1299 Mzimu mndipatseko,
  • Hymn 1190 Aleluya, mlemekeze,
  • Hymn 1012 Ndi zipatsozo,
  • Hymn 29 CHIKONDI cha
  • Hymn 1273 Ndasiya zonse ndi Yesu kalelo,
  • Hymn 1286 E, ndikukhulupirani,
  • Hymn 1143 Tikhale ndithu pomwepo;
  • Hymn 387 Tikutha kupemphera,
  • Hymn 1048 Kumwamba ndiona Ambuyangayo,
  • Hymn 60 ZATHEDWA zonsetu
  • Hymn 1530 Mndilimbitse ndipirire
  • Hymn 1230 Lichiza mzimu wophwetekwa ukakhale bata,
  • Hymn 812 Ndi ena sanamvera ‘yi,
  • Hymn 29 Tamandani Mbuye,
  • Hymn 1835 Mtima wanga lemekeza
  • Hymn 680 Mbendera yake ikupiza m’mlengalengamo,
  • Hymn 485 POMPANO pandikonda
  • Hymn 1468 Zobvala zake zonse
  • Hymn 1346 Ndaima pano, ndaima pakhomo:Lowa, lowa, lowa, lowa!
  • Hymn 344 M’watame,
  • Hymn 329 MUMZINDA wa Mulungu
  • Hymn 1663 Yesu Mbuye,
  • Hymn 463 Yesu atiuza tiwale ‘fe,
  • Hymn 307 ABALE anga ine ndikupita,
  • Hymn 220 MULUNGU mundichitire chifundo,
  • Hymn 352 Tiyamike Mlunguyo,
  • Hymn 330 Yesu ndiye Mtsogoleri
  • Hymn 245 Ngakhale kuthengo
  • Hymn 979 Limbikani inu nonse,
  • Hymn 1749 Chifukwa chipulumutso
  • Hymn 488 M’MANJA a Yesu wanga
  • Hymn 1152 Pokonda Yesuyo, mtendere!
  • Hymn 49 Ndi ife akudziwa
  • Hymn 388 MOMMUNO, Mbuye tionanetu,
  • Hymn 1197 Ndafoka ine kale,
  • Hymn 88 Ufuna kuwomboledwa kodi?
  • Hymn 206 Uzanitu abale,
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 543 Kuli kaphiri m’talimo
  • Hymn 275 NTHAWI yathu yafikatu,
  • Hymn 1521 Poyensedwa ife
  • Hymn 262 “KHALA mwa Ine,” Yesu anatero;
  • Hymn 1340 Perekani mtima wanu
  • Hymn 818 Mkhululukire,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 633 Tikasokera m’njira mutilondolere ndithu,
  • Hymn 1602 M’mawu a Yesu Mbuyeyo,
  • Hymn 1088 Mndiyandikitse nanu, Yesu,
  • Hymn 472 Amakumbukira zonse
  • Hymn 1809 Yampatsa Nowa yemwe,
  • Hymn 436 YEHOVA Mlungu wathu,
  • Hymn 249 Amen, Amen, Amen.
  • Hymn 737 Mommuno, Mbuye, tionanetu,
  • Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
  • Hymn 786 Yesu mkhale nafe
  • Hymn 1796 Ndikhulupira mwa Ambuye

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version