Skip to content

info@example.com

Treasure Hymns – Chichewa

  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service
  • About
  • Chichewa Believers Christian Hymns List
  • Chichewa Christian Hymns List
  • Contact
  • Home
  • Privacy Policy
  • Sample Page
  • Terms and Conditions
  • Terms of Service

Hymn 282 INU muli mehere,

  1. Home   »  
  2. Hymn 282 INU muli mehere,

Hymn 282 INU muli mehere,

December 14, 2025 treasurehymnsChichewa Christian Hymns

Chichewa Christian Hymns

Hymn 282 INU muli mehere,

 

INU muli mehere,
Wa dziko lapansi;
Ukasukuluka,
Sungakolerenso,

Yang’anani bwino,
Muyende m’njirayo;
Kuti mungagwetu,
M’zovuta za dziko.

Pamenepo sungakwanirenso kanthu,
Koma kuti ukaponyedwetu kunja.

Ndinu kuunika,
Kwa dziko lapansi;
Mudzi wapaphiri
Sungabisiketu.

Sungayatse nyali,
N’kuyivundikira;
Koma uyika pachoikapo chake.

Ndipo iwunikira onse
m’nyumbamo;
Chomwecho inu
muunikire dziko.

Kuti pakuwona,
Ntchitozo zabwino;
Alemekezedwe,
Mlungu ‘Tate wanu.

Post navigation

Previous: Hymn 281 MBUYE, mwatiuza ’fe
Next: Hymn 283 AMBUYE m’chipululu,

Leave a Reply Cancel reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Hymns You May Like

  • Hymn 1380 Tilemekezetu
  • Hymn 1852 Mbuye ndamva mwawazira
  • Hymn 1805 Anafa m’mvula muja
  • Hymn 756 Sindili woyenera ‘ne,
  • Hymn 986 Tiyeni anzathu
  • Hymn 36 AMBUYE tsopano lino, monga mwa mawu anu aja,
  • Hymn 1661 Ndimachitira
  • Hymn 1708 Pakugomedwapo
  • Hymn 76 E, MOYO wanga’we
  • Hymn 1526 Mbuye wondipulumutsa
  • Hymn 565 Koma sitimpenya m’khola
  • Hymn 1221 Bwenzi ndinamkomanayo,
  • Hymn 534 Bwerani, kondwerani,
  • Hymn 1157 Mtendere wapambana m’Mwambamo
  • Hymn 1636 Potuluka m’manda mwawo
  • Hymn 1645 Nafera inetu, nafera inetu
  • Hymn 903 Iwo salekana, iwo salekana,
  • Hymn 11 Imfa mutagonjetsa ndi zowawa,
  • Hymn 388 Ambuye, Mzimu wanu
  • Hymn 1363 Tamani Ambuye,
  • Hymn 1296 Chionerere mwaziwo
  • Hymn 1722 Ambuye tikondweratu
  • Hymn 834 Tiyamike Mlungu wotipatsa zachifundozi,
  • Hymn 430 Tero tidzakwera
  • Hymn 299 TIYENI, Akristu inu,
  • Hymn 1474 Zilepheradi zonse kugula moyowo,
  • Hymn 140 NDINAMIRA m’machimo, wosaonekanso,
  • Hymn 366 Anthu onse a padziko
  • Hymn 823 M’mwambamo nyenyezi
  • Hymn 115 Mbulu wanding’amba m’nthiti,
  • Hymn 987 Ambuye wa Kumwamba,
  • Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
  • Hymn 1588 Wandiwombola inetu
  • Hymn 1213 Mwamva Yesu m’mtimamo,
  • Hymn 1765 Zoonazi amithenga
  • Hymn 1630 Anthu anu amafoka,
  • Hymn 209 Mdima ufika, dzuwa lalowa,
  • Hymn 131 MAWU a Mulungu awa,
  • Hymn 452 Tiana ife tingofoka,
  • Hymn 1391 Ndiye wokondwa, E, munthuyo
  • Hymn 291 ULENDO wachikhrisitu ngosawutsa ndithu,
  • Hymn 1791 Tiimbe nyimbo zotamanda
  • Hymn 1204 Ambuyanga Yesu,
  • Hymn 553 M’munda muja ndaniyo
  • Hymn 372 Potero onsewo
  • Hymn 854 Timlemekeze Mlunguyu
  • Hymn 735 Mwa chikho chokumbutsa
  • Hymn 1424 Malo anachepa,
  • Hymn 1280 Kuti mundipatsa mphamvu yopambanayo;
  • Hymn 273 USAFUNE chuma chokha,
  • Hymn 469 NDIKONDA mbiri yomwe
  • Hymn 1817 Ndi m’munda muja chete, phee!
  • Hymn 21 KUZANI Mlungu m’Mwambamo,
  • Hymn 806 Kapena wina leroli
  • Hymn 470 YESU andikonda ine,
  • Hymn 98 YESU, Bwenzi la ochimwa,
  • Hymn 1576 Khamulo liliko
  • Hymn 1605 Yesu, dzina lokondwetsa
  • Hymn 218 NDIPEREKA zanga zonse
  • Hymn 271 Zoipa zangazi

Archives

  • December 2025

Categories

  • Chichewa Believers Christian Hymns
  • Chichewa Christian Hymns
  • Uncategorized
Proudly powered by WordPress | Theme: goldy-mex by inverstheme.
Go to mobile version